Chapita 15

1 Gabo yamalo yabanthu ba mtundu wa A Yuda, banja na banja, vkulila kumwela kumalile ya Edom, na cipulu ca zini kukhala kosilizila kumwela. 2 Malile yabo kumwela yambila kumapeto ya nyanja ya mucele, kucoka ku bay (nyondo) yoyang'ana ku mwela. 3 Malile yabo yotulikila kumwela wacikweza ca Akraboim nakupitila ku zin, na kuyenda ku mwela wa kadesh Barnea, munjila pa Hezroni, na pamwamba ku Addar, kwamene upindamukila ku karka. 4 Vnayendela ku Azmon, nakucokela pa musinje wa Eigipito, nakubwela kosilizila pa nyanja. Ndiye yanali malile yabo yaku mwela. 5 Malile yakumawa yanali nyanja ya mucele, pakamwa pa Yolodani. Malile ku mpoto yayambila pa bay (nyondo) ya nyanja pakamwa pa Yolodani. 6 Inakwela ku Beth Hoglah na kupitila munjila kumpoto wa Beth Arabah. pamenepo inakwela kumwala wa Bohan mwana wa Rubeni. 7 Ndipo malile yanakwela ku Debir kucokela kucigwa ca Achor, na ku mbali ya ku mpoto kupindamukila ku Giligala, yamene ili pafupi na phili ya Adummim, yamene ili kumwela kwa cigwa. Ndipo malile yanapitila ku mazi ya En shemesh na kuyenda ku En Rogel. 8 Pamenepo malile yanakwela pa cigwa ca Ben Hinnom ku mwela wa muzinda wa Ayebusi (yamene ni Yelusalemu). Ndipo pacigwa ca Hinnoni, ku mazulo, ya,ene ili posilizila kupoto ligwa ca Rephaim. 9 Pamenepo malile yanakulila kuyambila pamwamba pa phili kufika kumazi ya Nephtoah, nakucoka kuja kuyenda kumizinda ya phili ya Ephron. Ndipo Malile yakoneka mozungulukaku Baalah (cimo zi mozi monga Kiriath Jearim). 10 Pamenepo malile yazungulila kumazulo ya Baalah kuphili ya Seir, na kupitila munjila kumbali ya phili Jearim ku mpoto (cimozi mozi monga kesalon) inayendela pansi ku cetu shemeth, na kupitila ku Timmah. 11 Malile yanatulukila kumbali ya kumpoto ya phili ya Ekloni, na pamene munjila ya ku phili ya Baalah, kucoka paja inayenda ku Jabneel. malile ya nasilila panyanja. 12 Malile yakumazulo yanali nyanja yaikulu na malile yake ndiye malile yozongulila mtundu wa Ayuda, banja pa banja. 13 Mukusunga lamulo ya Yehova kuli Yoswa, Yoswa anapasa kalebu mwana wa Jephunneh malo pakati pa mtundu wa A Yuda, kiriath Arba, yamene, Hebloni (Arba anali tate ba Anak). 14 Kalebu anatuluka kucoka naba batatu ba Anak: sheshai, Ahiman na Yalmai; bana ba Anaki. 15 Anayenda kucoka kuja kukonka bokhala baku Debir (Debir inali kuitaniwa kiriath sepher). 16 Kalebu anakamba kuti, munthu wamene amenya kiriath sepher na kuitenga, kuli yeve nizapasa Aksah mwana wanga mukuzi monga mkazi wake.'' 17 Pamene Othniel mwana wa kenaz, mubale wa kalebu, anaitenga, kalebu anapasa iye Aksah mwana wake monga mkazi wake. 18 Mwamusanga Zitapita izo, Aksah anabwela kuli Othniel na kumuuza kuti apemphe munda kuli batate ake. pamene anaseluka pabulu wake, kalebu anakamba kuli yeve,'' ufumu cani? 19 Aksah anayankha,'' nipaseni daliso, popesa mwanipasa malo yakumwela: nipasesoni visime vamazi.'' pamene kalebu anampasa visime vapamwamba na pansi. 20 Ndiye cinali coloba ca mtundu wa Ayuda, banja pa banja. 21 Mizinda yakumutundu wa Ayuda kumaleke 10 ya kumwela, kufupi na malile ya Edom, yanali kabzer, Eder, Jagur, 22 Kinah, Dimonah, Adadah, Za 23 Kadesh, Hazor, Ithman, 24 Ziph, Telem, Bealoth, 25 Hazoh Hadattah, Kerioth Hezroni (iyi inali kuitawanso kuti Hazoh), 26 Amam, shem, moladah, 27 Hazar Gaddah, Heshmon, Beth pelet, 28 Hazar shual, Beersheba, Biziothiah. 29 Baalah, Iyim, Ezem, 30 Eltolad, Kesil, Hormah, 31 Ziklag, Madmannah, sansannah, 32 Lebaoth, shilhim, Aim na Rimmon, Aya Yanali mizinda twenti naini pamozi, kufakilako mizi yabo. 33 Mucigwa munali Ethtaol, Zorah, 34 Zanaoh, En Gannim, Tappuah, Enam, 35 Jarmuth, Adullan, Sokoh, Azekah, 36 Shaaraimu, Adithaim na Gederah. (yamene ni Gederothaim) Aya yanali mizinda fotini (14) pamozi, kufakilako na mizi yabo. 37 Zenah, Hadashah, Migdalgad, 38 Dilean, Mizpah, Joktheel, 39 Lachish, Bozkath, Egloni, 40 Kabbon, Lahmas, Kitlish, 41 Gederoth, Beth Dagon, Naamah, Makkedah. Aya yanali mizinda sikisitini (16) pamozi, Kufakilako na mizi yabo. 42 Libnah, Ether, Asha, 43 Iphtah, Ashnah, Nezib, 44 Keilah, Akzib, Mareshah. Aya yanali mizinda yalli naini (9) pamozi, Kafakilako mizi yabo. 45 Ekloni, namizinda na mizi zozungulila; 46 Kuyambila ku Ekloni kufika ku nyanja ikulu, na bonse benze kunkhala pafupi na Ashdod, kafakilako mizi yabo. 47 Ashdod, mizinda yozungulila, kafakilako mizi yabo; Gaza, mizinda yazungulila kufakilako mizi yabo; paka ku musinje wa Eigipito, na ku nyanja ikulu namalile yake. 48 Mu phili yaziko, shamir, Jattir, sokoh, 49 Dannah, Kiriath sannah (yamene ni, Debir), 50 Anab, Eshtemoh, Anim, 51 Goshen, Holon, na Giloh, Aya yana mizinda yali leveni (11) kafakilako mizi yabo. 52 Arab, Dumah, Eshani, 53 Janim, Beth Tappuah, Aphekah 54 Hvmtah, Kiriath Arah (yamene ni Hebloni), na Zior. Aya yanali mizinda yali naini (9) kafakilako mizi yabo. 55 Maon, Carmel, Ziph, Tuttah, 56 Jazreel, Jokdeam, Zanoah, 57 Kain, Gibeah, na Timnah, Aya yanali mizinda yali teni (10) kafakiko mizi yabo. 58 Halhul, Beth Zur, Gedor, 59 Manrath, Anoth, na Eitekoni. Aya yanali mizinda yali sikis (6), kafakilako mizi yabo 60 Kiriath Baal (yamene ni, Kiriath Jearim), na Rabbah. Aya yanali mizinda yabili, kufakilako mizi yabo. 61 Mucipululu, munali Beth Arabah, Middin, Scacah, 62 Nibshana, muzinda wa mucele na E Gedi. Aya yanali mizinda sikisi (6) kufakilako mizi yabo. 63 Koma kuli Ayebusi, bokhala mu Yelusalemu, mutindu wa A Yuda sanabacosemo, cifukwa cake Ayebusi akhala muja na mutundu wa Ayuda paka lelo.