Chapita 14

1 Aya ndiye mbali ya malo yamene bana Israyeli banalandila monga coloba cabo muziko ya kanani, yamene Eleaza wa nsembe, Yoswa mwana wa Nuni, na basogoleli ba mitundu yamabanja ya Israyeli anabagambila. 2 Coloba cabo cinasankhiwa na maele ku mitundu ili naini (9) na mutundu bogabika pakati, monga mwamene Yehova analamulila na zanja ya Mose. 3 Popeza Mose anapasa coloba ca mitundu ibilina mutundu vmozi bogabika pakati kupitilila Yolodani, koma kwa A Levi sanapase coloba. 4 Mutundu wa Yosefe yanali mitundu yabili, manase na Eflemu. A Levi sanapasiweko gabo yacoloba muziko, koma cabe mizinda yena ku khalamo, namalo ya vokudya ya vobeta vao na cuma cabo. 5 Bana ba Israyeli banacita monga Yehova analamulila Mose, ndipo banagawana malo. 6 Pamenepo mutundu wa Ayuda vnabwela kuli Yoswa pa Giligala. Calebu mwana Jephunneh mu kenizzite, anakamba kuli yeve,'' uziba zamene Yehova anakamba kuli Mose munthu wa mulungu pali iwe na ine pa kadesh Barnea. 7 Ninali nazaka fote pamene Mose mtumiki wa Yehova ananituma kucoka ku kadesh Barnea ukabona malo. Ni Nbwesa mau kuli yeve monga cinali mumitima mwanga kupanga 8 Koma abale banga banayenda naine banalengesa mitima yabanthu kusungunuka na manthu. Koma ine ndina konka Yehova mulungu wanga na mtima wanga. 9 Mose analumbila siku ija, kukamba kuti, zoona malo yamene mapazi yayendamo yazakhala coloba cako na bana bako nthawi zonse, cifukwa wakonka Yehova mulungu wanga namtima wako bonse. 10 Manje ona! Yehova anasunga namoyo izi zako fote faivi (45), monga mwamene anakambila - kucukela nthawi yamene Yehova anakamba mau aya kwa Mose, pamene Israyeli anayenda mucipululu. manje, ona! siku yalelo nili nazaka eite faivi (85). 11 Nikali na mphavu siku yalelo monga nenzeli musiku yamene Mose ananituma. mphavu zanga zili manje monga mwamene zinalilikale, za nkhondo, za kuyenda na kubwela. 12 Manje apa nipaseni iyi phili yaziko, yamene Yehova ananilonjeza pasiku ija. Popeza munamvela siku ija kuti ba Anakim banali kuja namizinda zikulu za malinga. cingakhale kuti Yehova azakhala naine nakuti nizaba cosamo, monga Yehova anakambila.'' 13 Oamene Yoswa anamudalisa na kumupasa Hebroni monga coloba kuli kalebu mwana wa Jephunneh. 14 Cifukwa cake Hebroni anakhala coloba cakalebu mwana wa Jephunneh mu kenizzite kufika siku yalelo, cifukwa anakonka Yehova, mulungu wa Israyeli na mtima wake bonse. 15 Manje zina ya Hebroni kali inali kiriath Arba. (Arba anali munthu mukulu pakati kaba Anakim) pamenepo malo yanapumula ku khondo.