Chapita 12

1 Manje aya ndiye mafumu yamuziko, bamene bamuna bamu Israyeli banagonjesa. Ba Israyeli banatenga malo kumbali yakumawa kwa Yolodani kwamene zuba icokela, kucoka kucigwa ca mumana wa Aroni kufka ku phiri ya Hermoni, na konse ku Arabah kumawa. 2 Sihon, mfumu ya Amoni, inankhala mu Heshbon. Anasogolela kucokela ku Aroer, yamene ili mumbali ya Arnon Gorge kucokela pakati ka cigwa, na pakati ya Gileadi kupita ku mumana wa Jabbok pamalile ya Amoni. 3 Sihon anajamulila pali Araban kufika kunyanja ya kinnereth, kumawa, kunyanja ya Arabah (nyanja ya mucele) kumawa! kuyenda ku Beth Jeshimoth na ku mwela, pansi poselukila phiri ya Pisgah. 4 Og, mfumu ya Bashani, mozi mwa opulumuka waba Rphaim, anakhala mu Ashtaroth na Edrei. 5 Analamulila pali phiri ya Hermoni, selekah, na konse ku Bashan, kumalile yabanthu ba ku Geshor na maacathites, na pakati ya Gilead, kumalile ya sihon, mfumu ya Heshbon. 6 Mose mutumiki wa Yehova, nabanthu ba Israyeli anabagonjesa, na Mose mtumiki wa Yehova, anapasa malo monga yabo kuli ba Alubeni, baGadites na pakati kamtundu wa manase. 7 Aya ndiye mafumu bamene Yoswa na banthu Israyeli banagonjesa kumbali yakumazulo kwa Yolodani, Kucokela ku Bar Gadi mucigwa pafupi na Lebanoni ku Phiri ya Halak pafupi na Edom. Yoswa anapasa malo kumitunda ya Israyeli kuti yakhale yabo beve. 8 Anabapasa mapili yaziko, ku cigwa, kumadimba, mbali yamapili, cipulu, na kumwela - malo ya ba Hittites, Amoni, Akanani, Apelezi, Ahivi, na Ayebusi. 9 Mafumu kufikilapo mfumu yaku Yeliko mfumu yaku Ai yamene ili pambali ya Beteli, 10 Mfumu ya Yelusalemu, mfumu ya Enaim, 11 Mfumu yaku Jarmuth, mfumu yaku Lachish, 12 Mfumu yaku Elgoni, mfumu ya ku Gezer, 13 Mfumu yaku Debir, mfumu yaku Gezer, 14 Mfumu yaku Hormah, mfumu yaku Aradi, 15 Mfumu yaku Libnah mfumu yaku Adullan, 16 Mfumu yaku Makkedah, mfumu yaku Beteli, 17 Mfumu yaku Tappuah, mfumu yaku Hepher, 18 Mfumu yaku Aphek, mfumu yaku Lasharoni, 19 Mfumu yaku Madon, mfumu yaku Hazor, 20 Mfumu yaku Shimron, mfumu yaku Akshaph, 21 Mfumu yaku Taanach, mfumu yaku Megiddo, 22 Mfumu yaku Kedesh, mfumu yaku Jokneam Carmei, 23 Mfumu yaku Dor mu Naphoth Dor, mfumu yaku Goyim mu Giligala, 24 Mfumu yaku Tirzah, Nambala yamafumu inafeti wai (13) pamozi.