Mutu 29

1 Pamene apo Yakobo anayenda paulendo wake na kufika ku malo ya bantu ba ku maba. 2 Pamene anayangana, anaona chisime mumunda, na, onani, magulu yatatu ya mbelele yanali gone mumbali. chifukwa cikuchoka mu chicime ichi banali kumwesalamo mbelele, na mwala unali pakamwa pachisime unali ukulu. 3 Pamene yonse magulu mbelele yanakumana paja, na bachibeta banali kuchosa mwala pakamwa pachisime na kupasa mbelele manzi, naku bwezapo chimwala futi pakamw pachisime, nakuchibweza mumalo yake. 4 Yakobo anakamba kuli benve kuti, "ba bale banga, mwachokela kuti?' bana yanka, "Tachokela ku Haran." Anakamba kuli benve, 5 "Mumuziba Labani mwana mwamuna wa Naha? "Nabenve banakamba kuti, "Timuziba. " 6 anakamba kuli benve kuti, "mwati alibwino?" Benve banakamba kuti, " alichabe bwino, na, yangananei kuja, Recho mwana wake mukazi abwela na mbelele." 7 Yakobo anakamba, "Onani, ni pakati pa siku. sintawi yama guli ya mbelele kukumana pamozi. mufunika kupasa mbelele manzi na kuyenda na kuzileka zidye." 8 Banakamba kuti, "sitinga zipase manzi mpaka zonse mbelele zikumane pamozi. Na bamuna baza chosa chimwala pachisime kuchoka apo tizazipasa manzi mbelele." 9 Pamene Yakobo anali kukamba na benve, Recho ana bwela na mbelele zaba tate bake, chifukwa niwamene anali kuzibetela. 10 Pamene Yakobo anaona recho, mwana mukazi wa Labani, mubale wa bamai bake, na mbelele za Labani, mubale wa bamai bake, Yakobo ana bwela pamene paja, naku vendesa mwala kuchoka pakamwa pachisimenakupasa manzi gulu ya mbelele za Labani, mubale wa bamai bake. 11 Yakobo ana pyopyonta Recho nakulila mo kuwa. Yakobo anauza Recho, kuti enve anali bululu wa batate bake, anali mwana wa Rabeka. 12 Pamene apo enve anatmnaga na kuyenda ku'uza batate bake. 13 Pamene Labani ananvela iyi nkani ya Yakobo mwana mwamuna wamulonosi wake, anatamanga kuti bakumane na enve, na kumukumbatila, na kumu pyopyonta, na kumu bwelesa ku nyumba yake. Yakobo anauza Labani vonse ivi vintu. 14 Labani ana kamba kuli enve, "iwe zo'ona ndiwe fupa yanga na munofu wanga." ndiye pamene Yakobo ana nkala na paka ntawi ya mwezi umozi. 15 Ndiye pamene Labani anakamba kuli Yakobo kuti unga ni sebenzele mahala chifukwa ndiwe bululu wanga? Niuze, malipilo yako yazankala bwanji?" 16 Manje Labani enzeli na bana bakazi bali. Na zina ya mukulu yenze Leya, na zina ya mungono yenze Recho. 17 Menso ya Leya yanali yofewa, koma Recho anali okongola, mukapangidwa nama onekedwe. 18 Yakobo anakonda Recho, ndiye chamene anakambila, "nizaku sebenzelani zaka seveni ya Recho, mwana wanu mun'gono mukazi. 19 Labani anakamba kuti, "nicha bwino kuti ine nipupase enve kuli iwe, osati ine nipase enve kuli mwamuna wina. nkala na ine." 20 Na Yacobo anasebenza zaka seveni ya Recho; koma yanamuonekela kwati nimasiku yangono, chifukwa cha mwanen ana mukondela. 21 Pamene apo Yakobo anakamba kuli Labani, "nipase ine mukazi wanga, chifukwa masiku yanga yakwanila kuti nimukwatile!" 22 Manje Labani anaitana pamozi bantu bonse ba pamalo nokupanga pwando. 23 24 25 Mumazulo, Labani anatenga Leya mwana wake mukazi nakumubwelesa enve kuli Yakobo, wamene anangena muli enve. Labani anapasa wanchinto mukzai Zilpankuli mwana wake mukazi Leya, kunkala wanchonto ake. Kuseni, onani, enze Leya! Yakobo anakamba kuli Labani, "nanga ndiye vichani vamene wa chita kuli ine? nanga ine sinina sebenzele Recho? Nichifukwa cha chani mwani nama ine?" 26 Labani anakamba, simwambo watu kupasa mwana mukazi mungono tikalibe kupasa mwana mukulu. 27 Silizisa mulingu wa uy mwana mukazi, koma tizakupsa na winangu monga malipilo pakuni sebenzela zaka seveni zinangu." 28 Yakobo anachita sochabe, naku siliza mulingu wa Leya. Ndiye pamene Labani anamupasa Recho mwana wake mukazi kunkala mukazi wake an enve. 29 Labani ana pasa Bilhah kuli mwana wake mukazi Recho, kunkala wanchito wake. 30 Na Yakobo anangena muli Recho, na enve, koma ana konda Recho kupambana na Leya. Na Yakobo anamusebenzela Labani zaka zinangu zili seveni. 31 32 Yehova anaona kuti Leya sanali okondewa, anasegula mala yake, koma Rcho analibe mwana. Leya anankala namimba nakubala mwana mwamuna, nakumu itana ina Rubeni. chifukwa anakamba kuti, "Chifukwa Yehova ayangana paku vutika kwanga; zo'ona apa maje bamuna banga bazani konda ine. 33 Ndiipo anakahala namimba futi na kubala mwana mwamuna. Ana kamba, "Chifukwa Yehova anvela kuti sindine okndewa, anipasa futi mwana mwamuna."Ana mupasa zina Simioni. 34 Anankhala futi namimba nakubala mwana mwamusa. Anakamba, "apa manje bamuna banga bazangwilikana kuli naine, chifukwa naba balila bana bamuna batatu."Chaicho anaitaniwa zina ya Levi. 35 Ankhala na mimba futi nakubala mwana mwamuna anakamba, "ino ntawi nizamutamanda Yehova. Ndiye pamene apo ana mu itana zina yake Yuda; ndipo analaka kunkala na bana.