Mutu 26

1 Ndipo kunali mu ziko, kumbali kwanjala yoyamba yamene ina chitikka muma siku ya Abrahamu. Isaki anayenda kuli Abimeleki, mfumu yaba Aphistini ku Gela. 2 Manje Yehova anaonekela kuli eve naku muuza kuti, "usayende ku Egypito; nkala mu ziko yamene nakuuza kunkala. 3 Nkala mwamene muno mu zika. Ndipo niza nkala naiwe naku kudalisa iwe; kuli iwe naku bobadwa muli iwe, nizakupasa ma ano chamene ninalapila kuli Abrahamu tate wako. 4 Nizapakisa bobadwa mwa iwe monga nyenyezi za kumwamba, ndipo nizapasa kuli bobabdwa mwa iwe maziko yonse ayakupitila muli iwe maziko yonse ytapansi yazadalisika. 5 Nizachita ichi chifukwa Abrahamu ananvelele mau yanga nakusunga malangizo yanga, lamulo langa, malemba yanga, na malamulo yanga." 6 Ndipo Isaki anankala ku Gerari. 7 Pamene bazimuna bana funsa pali mukazi wake, anakamba. "Nimulongo wanga." ananvela mantha kukamba, "Nimu kazi wanga," chifukwa enzekuganiza, bazimuna bakuno ku malo bazani paya kuti batenge Rabeka, chifukwa niwabwino." 8 Pamene Isaki anakalako maningi kuja Abimelelki mfumu wabo ba Philistini ana sonjela pa (Zenela). Anayanga onani, Isaki anali ku gwila Rabeka, mukazi wake. 9 Abimeleki ana muitana Isaki kuli eve ana muza, "Ona, Zoona nimukazi wako chifukwa nichani unakamba kuti nimu longo wako?" Isaki ana muza eve, "chifukwa nenze kuona monga wina angani paye kuti amu tenge." 10 Abimeleki anakamba, " Nichani ichi chamena wachita kuli ise? Cinali nichapafupi kuti umozo wabantu agone namukazi wako, ndipo sembe watiletela kuchimwa pali ise." 11 Ndipo Abimeleki anaba Chenjeza bonse bantu naku bauza, "Aliyense wamene azangwila uyu mwamuna olo mukazi wake zoona azapaiwa." 12 Isaki anashanga mbeu mu ziko muja naku kolola muchaka chamene kali handredi cifukwa Yehova anamudalisa. 13 Anankala mwamuna wolemela, ndipo anankala wolemela ndi kulemela paka anankala wolemela maningi. 14 Anali na mbelele na ng'ombe zambili nabanja ukulu. Ba Philistini bana mukumbwila. 15 Manji visime vonse namene banchito batate bake banakumba mumasiku ya Abrahamu tate wake, Ma Philistini bana vilekesa mwaku vifwikala na doti. 16 Abimelelki anamuza Isaki, "Yenda coka kuli ise, pakuti ndiwe wampavu maningi kuchila ise." 17 Ndipo Isaki anachokako kuja nakunkala muchifwa ua Gerari, nakunkala mwamene kuja. 18 Koma futi Isaki anafukulula visime vamanzi, vamene vinakumbiwa mu masiku ya Abrahamu tate wake. Ba Philistini benze bana vifwikila kuchokela pa infa ya Abrahamu. Isaki anavipasa visime ma zina yamene batate bake banali kuvitana. 19 Pamene banchito ba Isaki banakumba chigwa bana peza kuja cisime chamanzi yoyenda. 20 Bamuna bobeta baku Gerari bana yambana na muna bobeta ba Isaki, ndipo banakamba, "aya nimanzi yatu." ndipo Isaki anaitana cisime "Eseki," cifukwa abayambana nayeve. 21 Ndipo bana kumba cisime cinangu, ndipo bana yambana pali icho, futi, ndipo anachitana anachipasa zina "Sitina." 22 Anachoka kuja ndipo anakumba futi cinangu cisime, koma sibana yambana pali ici. ndipo anachitana Tehoboti, nakukamba kuti. "Manje Yehova ati pangila malo ise, ndipo tiza tukuka mu ziko. 23 Kuchoka apo Isaki anachokako naku yenda ku Beereseba. 24 Yehova anamuokela usiku wamene uja nakukamba, "ndine Mulungu wa Abrahamu tate wako usayope, pakuti nili naiwe ndipo niza kudalisa iwe naku chulukisa bobadwa muli iwe chifukwa cha Abrahamu wa nchito wanga. 25 Isaki anamanga guwa kuja na kuitana pa ziko ya Yehova. Kuja ana kokomela hema, ndipo banchito bake bana kumba cisime. 26 Ndipo Abimeleki anayenda kuli eve kuchokela ku Gerari, na Ahuzzati, na mu zake, na Phico, mukulu wa ba silikali. 27 Isaki anabauza, nichani mwabwelela kuli ine pakuti muni zonda ndipo muna nipisha kuchoka kuli imwe?" 28 Banamuyanka kuti zoona taona kuti Yehova alina iwe. Ndipo taganiza kuti pankale kulapila pakati patu pakati patu na iwe. Manje tiyeni tipange chipangano naiwe, 29 kuti silizatichita ise choipa, monga mwamene ise sitinaku chite voipa, monga mwamene tinakusungila bwino nakulaila mwa mutendele. Zoona, ndipo odalisika na Yehova." 30 Ndipo Isaki anabapangila pwando, ndipo bana dya naku mwa. 31 Bana uka kuseni maningi naku lumbila kuli wina namu zake. Ndipo Isaki anaba laila, bana musiya mu mtendele. Siku yamene chisime shiba, ndipo zina ya muzinda uja ni Beershiba paka siku yalelo. 32 Siku yamene ija wanchito wa Isaki anabwela naku muuza pali chisime chaene bana kumba. Bana kamba "Tapeza manzi." 33 Anachitana chisime shiba, ndipo zina ya muzinda uja ni Beershiba paka siku yallelo. 34 Pamene Esau enze na zaka fote, anatenga mukazi, Judi mwana wa Beeri waku Hittiti, naye basimati mukazi wa Eloni waku Hitti. 35 Banaleta misozi kuli Isaki na Rabeka.