Mutu 23

1 Sarai anankhala zaka 127. Izi ndiye zaka zawumoyo wa Sarai. 2 Sarai anafela mu Kiriti Arba, ndiye kuti, Hebroni, muziko ya Kenani. Abrahamu ana dandaula na kulila Sara. 3 Pamene apo Abrahamu anayamuka na ku cokako kwa mukazi wake wokufa, na kunena ku bana ba A'Heti, kuti, 4 " Ndine mulendo pakati panu. Nipasenikoni malo ya manda pakati pa imwe, kuti ni ike wanga okufa. 5 Wana wa Heti bana muyankha Abrahamu, kuti, 6 " Tiveleni ife, bwana wanga. Ndimwe mwana wa mfumu wa Mulungu pakati katu. Ikani wokufa wanu mumanda yathu ya bwino. Kulibe amene azakulesa manda yake, kuti uyikemo wa kufa wako." 7 Abrahamu ananyamuka naku gwanda kubantu amudziko, kuli bana A'Heti. 8 Iye anakamba nabo, kuti ngati imwe mwavomela kuti n ike bokufa wanga, manje ninveleni na kunimpepelako kuli Efulon mwana wa Zohari, kuli ine. 9 Muni funsileko kuti aningulise kavu ya Machipela, yamene alinayo, yamene ili kumapeto yakumunda wake. Pa mutengo wake wonse, anigulise powonekela ngati malo yoyikapo ba kufa." 10 Isapano Efroni anali anankhala pakati pa bana ba Heti, ndipo Efroni Mhiti anayanka Abrahamu mu manso ya bana ba Heti, na bonse bamene bana bwela mu geti yamu zinda wake, kuti, 11 iyayi, bwana wanga, niveleni ine, naku pasani munda, na kavu yamene ili mukati. Nakupasa iwe pa manso ya bana ba banga. Nakupasa iwe kuti uyike okufa wako." 12 Pamene apo Abrahamu anagwanda pa manso pa bantu a mudziko. 13 Anakamba na Efron mukuvelela kwa bantu bamu dziko, kuti, koma ngati mufuna, napapata niveleni. Nizalipila zamunda. Tengani ndalama kuchokela kuli ine, ndipo niza ika wokufa wanga kuja." 14 Efron anayankha Abrahamu, kuti 15 " Chonde, bwana wanga, niveleni ine. Ka malo ka nthaka ko kwanila muyeso wafolo handredi ma shekeli ya siliva, ni cani ici camene cili pakati pali ine na iwe? Ika wakufa wako." 16 Abrahamu anavelela kuli Efulon ndipo Abrahamu ana pimila Efulo muyeso wa siliva wamene ana tomola pokamba milandu nabana bamuna ba Heti, Folo handiledi ma shekelo ya siliva, kulinga na kapimidwe ka bwino kama londa. 17 Munda wa Efulon, wamene unali mu Machifela, wamene unali pa fupi na mamre, uyo ndiye yonse yamene inali mu munda na konse muma lile, vina pasiwa 18 Bana vingulisa kuli Abrahamu pa manso ya bana bamuna ba Heti, pali bonse bamene benze bana bwela mu geti ya mu zinda wake. 19 Pasongolo pake, Abrahamu ana yika thupi ya Sara mukazi wake mu kavu ya mu munda wa machipela, wamene uli pafupi na Mamre, uyu ndiye Hebloni, muziko ya Kanani. 20 Ndipo munda na kavu vinalimo vina pasiwa kwa Abrahamu kuti vinkhale katundu wake woyikilamo malilo, kucokela ku bana ba muna ba Heti.