Mutu 16

1 Manje Sara, mukazi wa AAAAbrahamu, sana mu barile mwana eye, koma anali na wacito mukazi. Munthu waku Ejipito, wamene zina yake Aga. 2 Ndipo Sara ana kamba na Abulahamu. ' Ona, Yehova anigwila ene kusakhala na bana. Enda uka gone na wacito. Ciga nkale kuti nizankhala na bana mwa eye." Abulahamu anavela ku mahu ya Sara, 3 pamene Abrahamu anankhala zake 10 mukanani pemozi na Sara, mukazi wa Abulamu, ana pasa aga, wacito wake waku Ejipito, mwa muna wake ku nkhala mu kazi wake. 4 Sopano anli chibwezi na Aga, ndipo anankhala namimba. Pamene ana ona kuti ana kuti ankhala namimba. Ana nkhala na chifukwa na omulemba wachito wake. 5 Ndipo Sara anakamba na Abrahamu, " Uku kulakwa kwanga chifukwa cha ewe. Ni nakupasa wachito wanga mukazi kuti ukale naye, pame anaona kuti ankhala namimba omulemba chito wake. Sinina muko dwelese mu maso yake. Leka Yehova a weluze pakati paine na ewe. 6 Koma Abulamu anakamba kuli Sara, " Ona pano, wachito wako muzimai ali mu manja yako. Chita na eve chimane uganiza uza ku wamiza. " Sopano Sara ana chita mwankhaza na eve, ndipo anataba kuchoka kwa eve. 7 Mu ngelo wa Yehova ana mupeza mu bali ya manzi muchipululu, mu bali ya mumanzi pajila Suri 8 Ana kamba, " Aga, wachito wa Sara, uchikelekuti ndipo uyenda kuti? " Ndipo ana yanka kuti, " Nili kutaba kuli unilemba chito wanga." 9 Mu ngelo wa Yehova ana kamba nae. " Bwelela kuli okulemba chito wako. Zipeleke na kuzi chepesa ku ulomulilo wake." 10 Ndipo mu ngelo wa Yehova ana kamba nae, " ni zaku chulukisa kwabili obabadwa kwaiwe. Kuti ba ka khale bubili ochuka osabelengeka." 11 Mu ngelo wa Yehova anakambaso naye. " Onani, wankala na mimba uzakara na mwana mwamuna. Ndipo uza mu etana Zina Ishemaeli. Chifukwa Yehova a vera kuvutisika kwako. 12 Aza nkhala munthu. Ngati bulu wamu sanga, azakhala osa velana na munthu aliyese, ndipo aza siyana naba bale wake." 13 Ndipo anapase zina iyi kuli Yehova wamene kamba naeye, "Ndiwe Mulungu wamene uniona ine," ndaba ana kamba, " Kodi ne pitiliza ku ona, ngankhale pa buyo poni ona ene? " 14 Kwaichoo chi ceme china itanidwa Beaya Roi, Onani, chili pakhati Kadesh ndi Beredi. 15 Aga ana bara mwana mwamuna kwa Abramu, ndi Abramu anamupa zina mwana wake mwamuna wamene Aga anamu barila, Ishmaeli. 16 Abrahamu anali ndi zaka Eite sikisi pamene Aga ana bara Ishmaeli kwa Abramu.