Mutu 15

1 kuchoka apa mau ya Yehova yanabwela kuli Abulam mumasomphenya, kukamba kuti, "Usa yope, Abramu! ndine wokuchingilila ndipo ndine mphoto yako yaikulu." 2 Abramu anakamba kuti, "Ambuye Yehova, muzanipasa chani, pakuti nilibe mwana, ndipo oloba nyumba yanga ni Elyeza waku Damasicus?" 3 Abramu anakamba kuti, "Pakuti simunanipase mwana, onani, umozi obadwa munyumba yanga azankhala oni loba!" 4 Ndipo, onani, mau ya mulungu yana bwela kuli eve, kukamba, "Uyo munthu saza nkhala oloba waku; koma wamene azachokela kuthupi yako ndiye wamene azankhala oloba wako." 5 Ndipo anamubwelelsa panja, na kukamba, "Yangana kumwamba, na kupenda nyenyezi, ngati unga kwanise kuzipenda." Ndipo namuuza kuti, "Ndiye mwamene obadwa mwaiwe bazankhalila." 6 Anakhulupilila Yehova, ndipo chinapendeka kuli eve monga chilungamo. 7 Anamuuza iye kute, "Ndine Yehova, wamene anakuchosa mu Uri wa Achaudini, kukupasa malo aya kuti ulobe." 8 Anakamba, "Ambuye Yehova, nizaziba bwanji kuti chizankhala choloba changa?" 9 Ndipo anamuuza kuti, "Niletele ng'ombe ikazi yazaka zitatu, mbuzi ikazi yazaka zitatu, nambelele yazaka zitatu, nkhunda, nanjiba. 10 anamulete zonse, ndiku yang'amba pa bili, ndiku vifaka vi langanana, coma sana patulisane nyoni. 11 pamene vi nyoni vinabwela pansi pama tupi ya nyama yokufa. Abramu ana vi pisha. 12 Ndipo pamene zuba inali kuyenda pansi, Abramu anagona tulo ndipo, onani, vonse vi nali pafupi naye vinakhala mudima ndiku yofya. 13 Ndipo Yehova anati kwa Abramu,"ziba kuti bobadwa pa mboyo pako bazankhala alendo pa malo yamene si ili yabo, ndipo banhkala mukapolo ndi ovutisiwa. 14 Nizaweluza calo chija camene bazasebenzela, ndipo kuchoka apo baza choka na vinthu vambili. 15 coma muzayenda ku malo yaba tate banu mu mutendere, ndipo muzashikiwa zaka za bwino zaunkhalamba. 16 mubadwo wa nambala fo baza bwela futi, po peza machimo yama Amoni yakalibe kufika pama lile,". 17 Pamene zuba inangena ndipo kwenze mudima, onani, poto yenze na chusi ndi nyali yo yaka pakati kama duswa. 18 Pasiku ija Yaweh anapanaga chipangano na Abramu, kukamba kuti, "Kuli bonse bamubadwe bako naba pasa malo aya, ku chokela kumumana wa Iguputo kufikila kumumana yampamvu, Yufurate- 19 ma Kenetes, ma Kenezete, ma Kadomonetes, 20 ma Hittetes, ma Perizzites, ma Refates, 21 ma Amorites, Canaanites, ma Girgashites, na ma jebutes."