Mutu 14

1 Inofika nthawi ya masikhu ya Amlafelo, mfumu ya ku shima, alioki, mfumu ya elasa, kedalama mfumu ya elamu na fidolo, mfumu yaku Goimu, 2 Mpaka ba namenya nkondo yo kangana na Bela, mfumu yaku Sodomu. Besha, mfumu ya Gomola. Shimabu, mfumu ya Adimo, Shemeba, mfumu ya Zeboyimu, na Bela, mfumu, ( wamene baitana kuti Zoa). 3 Aba bakusogolo mafumu yo kwanla faivi ana gwilizana pa modzi mu malo ya marizi yaku Sidimu, (yamene baitana kuti kite nyanja ya sauti). 4 Zaka zokwanila twobvu bamali ku Sebejela kedalaoma, khoma mu chaka cha sateni bana mu ukila. 5 Ndiponso mu chaka cafotini, kedalama na mfumu zinali na eve zina bwela ku menya lefaimu mu Ashifaloti Kamoimu ma zuzitesi mu Hamu, ba Emitesi baku shave Kiliataimu. 6 Na ba Holitesi mu mapili yaku mapili m'calo caku Sega, polingama ku talipa monga elo palari, yamene ili pafupi na dezeti. 7 Ndiposo ba nabwelela ndi kufika ku Eri mushipati, ( yamene baitana futi kuti Kadeshi), naku gonjesa calo conse ca ku Amolekaitesi, ndi ba Amolaiti benza nkala ku Hazezoni Tamah. 8 Ndiponso mfumu yaku Sodomu, mfumu yaku Gomola, mfumu ya Adama, mfumu ya zeboyimu, na mfumu yamu Bela (yamene boitana futi kuti Zoa) anayenda panja na ku konzelekela nkondo yaku malo ya manzi yaba Sidimu. 9 Mokangana na Kedalaoma, mfumu mfumu yaku Elamu. Tido, mfumu yaku Goimu. Amulafelo, mfumu yaku shina Nioki, mfumu elasa, mfumu zili folo zina kangana na zili faivi. 10 Apa manje m'chigwa ca Sidimu m'nali mo zula ndi migodi ya manenekela, ndipo mfumu zaku sodomu naku Gomola pamene zinali kutaba, zinagwelamo. Ba mene banasala banataba ku ma pili. 11 Apa mafumu yamatenga katundu yonse yaku Sodomu na Gomola mangonse zofumkila kuli beve ndipo bana bwelela kwamene bana chokela. 12 Pamene bana enda bana tenga na Loti, mwana anabadwa kuba m'bale wa Abramu, wamene anali ku nkala ku Sodom, pamozi nazeke zonse. 13 Ndipo umozi anapulumuka anam'bweza kuyenda ku udza Abramu mu Hebeli. Wamene anali kunkala pakati pa mitengo yaku mamule, mu Amolite, anali m'bale wa Eshukolo na ana, bonse pamodzi banali kumbali ya Abramu. 14 Apo pamene Abramu anavela kuti bodani bagwila mbululu wake, anasongolela amuna bopuzisiwa bo nkondo bobodwila mu banja yake bokwana 318, ndipo anapisha bodani m'paka ku Dani. 15 Iye ana gabanisa bantu bake bamuna usiku nakuyamba ku menyana nawo, naku bapisha m'paka ku Hoba, yamene ili ku m'polo kwa Damasikasi. 16 Ndipo anabwela na zafunikila zonse, na m'bululu wake Loti nazake gonse, na bazimayi na banthu benangu. 17 Pamene Abramu anabwelela kugonjesa Kedalaona na ma mfumu yanali kumbali yake, mfumu yaku Sodomu ina yenda kukumona naye ku maloya chigwa ku shave ( yamene ba itana kuti malo ya chigwa ca mfumu). 18 Melekizedeki, mfu yaku Salemu inabwela na mukate na vinyu. Anali wanaembe wa Mulungu wamukulu. 19 Ana mudalisa eve pokambakuti, " Adalisike Abramu na Mulungu wake wamu mwamba, wamene analenga ku mwamba na ziko lapansi. 20 Adalisike Mulungu waku mwamba mwamba, wamene anakupasa badam bako m'kwanja mwako." Kuchoka apo Abramu ana mupasa chakumi pa zonse zake. 21 Mfumu yaku Sondomu inakamba kuti Abramu ati, " Nipase bantu, koma tenga katundu yonse niyako." 22 Abramu anakamba kwa mfumu yaku Sodomu ati, " Nanyamula manja ku mwamba kuti yawe, Mulungu waku mwamba mwamba, wolenga ziko yaku mwamba napansi. 23 Kuti sinizatengapo kantambo, olo kamagila nsapato, kapena chili chonse cako, kuti usakakambepo, 'Ati ninamulemelesa Abramu.' 24 Sinizalenga chili chonse kuchosako chabe vamene anyamata ba ny'ono bany'ono banadiya ndiponso mbuli ya nyamata amene ananipelekeza. Lekani Aneli, Esikolo na mamile dengepo mbali yawo.