Mutu 3

1 Manje kunali nkondo yopitilila pakati nyumba ya Saulo na nyumba ya Davidi. Davidi na limba ku limbilatu koma nyumba ya Saulo ina faka ku fokelatu. 2 Bana bamuna banabadwa kwa Davidi ku Heberoni. Mwana wake oyamba anali Amnoni, kuli Ahinoami waku Jezereli. 3 Mwana wake wachibili mwamuna, Kileabu, anabadwa kuli Abigail, ofedwa wa Nabo waku Kameli. Wachitatu, Absalomu, ana mwana wa maaca, mwana mukazi wa Tamai, mfumu ya Geshuri. 4 Davidi mwana mwamuna wa namba fo, Adonija, anali mwana wa Haggaiti, mwana wake wa namba faivi anali Shefatiia mwana wa Abita, 5 na wachi sikisi, Itreamu, anali mwana mwamuna wa Davidi mukazi wake Elga. Bana bamuna bana baddwa kuli Davidi ku Heberoni. 6 Zina chitika pamene pakati pa nkondo nyumba ya Saulo na nyumba ya Davidi kwakuti Abnei ana zilimbisa mi nyumba ya Saulo. 7 Saulo anali na mai nini wamene zina yake yenzeli Rizpa, mwana mukzai wa Ayia. Isiboseti anakamba kuli Abneri, "chifukwa chani wayenda kuli bamai nini baba tate banga?" 8 Pamene apo Abneri anakalipa kwambili pa mau ya Isiboseti naku kamba kuti, "kodi ndine mutu wa yayimbwa yaku Yuda? Lelo Ine nilangizani kukalipa ku nyumba ya Saulo, batate bako, kuli bale bake, na kuli banzake, kamba kosa kupeleka iwe mumanja ya Davidi. Koma manje uninamizila ine mulandu kwa muzimai uyu? 9 Mulungu achite ine, Abneri, na mopambanaso, ngati siniza chita kwa Davidi ngati Yehova ana lubila kwa iye, 10 kuchosa ufumu ku nyumba ya Saulo naku ika mpadno kuli Davidi kuli Isilayeli na pali Yuda, kuchokela kwa Dani kuli Beersheba." 11 Isiboseti sana muyanke Abneri mau yena, chifukwa ana muyopa enve. 12 Pamene apo Abneri anatuma tumiki kuli Davidi kuzi kambila iye yeka kuti, "Ni malo yandani aya? panga chipangano nainee, ndipo uzaona kuti kwanja yanga ili na iwe, kuleta bonse ba Isilayeli kwa iwe." 13 Davidi anayanka kuti, "kwabwino, nizapanga chipangano na iwe. Koma chimozi izafunka kwa iwe nikuti suzaona nkope yanga pokampo choyamba leta Micha, mwana mukazi wa Saulo, uka bwela kuniona ine." 14 Pamene apo Davidi anatuma ntumi kuli Isiboseti, mwana mwamuna wa Saulo, kukamba kuti, "nipase ine mukazi wanga Mizha, wamene nina lipilila mutengo wa wani handiledi Afilisiti mudulidwe wabo." 15 Chakuti Isisobeti anaitansia Micha na kumu chosa enve kuli mwamuna wake, Paltieli mwana mwamuna wa Laishi. 16 Mwamuna wake anayenda na yenve, molila pamene enze kuyenda, ana mukonka enve ku Bahurimu. PAmene apo Abneri ana kamba kuli enve, "bwelela kunyumba manje." ndipo ana bwelela. 17 Abneri anakamba naba sogoleli ba Isilayeli kukamaba kuti, "siku ya kumbuyo una yesa kumutebga Davidi ku nkala mfumu paiwe. 18 Manje chichite. Kamba Yehova akamba na Davidi kukamba kuti, na kwanja ya wanchtio wanga Davidi niza pulumusa bantu banga Isilayeli kuchokela ku manja yama Filisiti naku chokela ku manja yaba ndani babo."' 19 Abneri ndipo anakamba paiye yeka ku bantu baku Benjameni. Pamene apo Abneri anayendaso kukamba na Davidi ku Heberoni kufotokoza vonse va Isilaye;li na nyumba yonse ya Benjameni kufunisisa ku kwanisil. 20 Pamene Abneri na bantu bake twenty babfika ku Heberoni kuona Davidi, Davidi anali na pwando yokonzekela benve, 21 Abneri ana mufotokozela Davidi, "Nizanyamuka naku sonkanisa bonse ba Isilayeli kwaiwe, bwana wanga mfumu, kwakuti bapange chipangano naiwe, kwakuti uka lamulie vonse vamene iwe wakalaka." Chakuti Davidi anatuma Abneri kuyenda, ndipo Abneri anayenda mwa mutendele. 22 Pamene apo basilikali ba Davidi na Jowabu bana bwelela kuchokela ku nkondo yobvumbulukila naku nkala nazo zofunikila vambiri koma Abneri sanali ku Heberoni kwa Davide. Davidi anamupisha enve, ndipo Abneri anayenda mwa mutendele. 23 Pamene Jowabu naba silikali bonse banfika na enve, bana mu'uza Jowabu, "Abneri mwana wa Neri anabwela kuli mfumu, ndipo Abneri anayenda mwamutendele." 24 Pamene Joabu anabwela kuli mfumu naku kamaba kuti, "Wachita chani? kuli Abneri anabwela kuli iwe! Nichani wamuoisha, ndipo ayenda? 25 Kodi iziba kuti Abneri mwana wa Neri enzeli anabwela kuku namiza iwe na kuziba malingililo na ziba zonse zamene uchita?" 26 Pamene Joabu anamusiya Davidi, anatuma ntumi kuli Abneri, ndipo bana mubwalisa futi kuchoka ku chicime cha Sira, koma Davidi sanab vizibe enve. 27 Pamene Abneri ana bwelela ku Heberoni, Joabu ana mutenga pa bali pakati pa chiseko ku kamaba naye mwaka chetecheta. Kwamene kuja Joabu ana mulasa mamala na kumupaya enve. Munjila iyi, Joabu ana bwezala magazi ya Ashaheli mubale wake. 28 Pamene Davidi ananvela ivi anakamba kuti, ine na ufumu wanga ndise ba kayele pamenso ya Yehova muyaya kulingana na magazi ya Abneri mwana wa Neri. 29 Lekani magazi yake ya gwele pa mutu wa Joabu napa nyumba ya Joabu tate bake! Lekani nyumba ya Joabu pasaka sobe muntu alina vilonda pa nkanda mwina olemala ndipo afunika kuyenda na ndondo mwina wamene apaiwa na mupeni mwina kupeleka chakudia." 30 Chakuti Yowabu na Abishali mubale wake ana mupaya Abneri, chifukwa anali anapaya mubale wabo Asaheli ku Gibiyoni ku nkondo. 31 Davidi anakamba kuli Joabu ankuli bantu bonse banali na enve, "Ngambani vovala vanu, valani vovala vama saka, ndipo mulile pamenso pa tupi ya Abner." Manje mfumu Davidi anayenda kumbuyo ya tupi m ntawi ya malilo. 32 Bana mushia Abneri mu Heberoni, Mfumu inalila naku punda monveka pa manda ya Abneri, ndipo bantu bonse nabo bana lila. 33 Mfumu ina mulila Abneru na nyimbo, kodi Abneri okufa monga vipuba mwamene vifela? 34 Manja yako siyenze yo mangiwa. Mendo yako siyneze yo mangililwa. Monga muntu wakugwa na bantu oyipa, mwamane una iwe." ndipo bantu bonse bana mulila enve. 35 Bantu bonse bana bwela kudyesa Davidi pamene kukali muzuba. Koma Davidi analubila, "Mulungu achite naine manje, ndipo mopitililanso, ngati niza laba mukate mwina chilichonse pamene zuba ikalibe kungena pansi. 36 Bantu bonse bana zindikila kubabiwa kwa Davidi, ndipo chinaba nkodwelesa benve, vili vonse mfumu vamene ina chita vinaba kondwelesa benve. 37 Chakuti bantu bonse na Isilayeli yonse bana nvesesa inja siku kuti chiche nali chifunilo cha mfumu kupaya Abneri mwana wa Neri. 38 Mfumu ina kamba kuli wanchito wake, "Kodi uziba kuti mwana mfumu na muntu mukuru agwa mu Isilayeli? 39 Manje ndine ofoka lelo, nga nkale ndine mfumu yo zozewa. Aba bantu, bana ba aZeruiaha, niba kanza kwa ine. Lekani Yehova aba bwezele voipa vabo, monga ayenila enve."