Mutu 2

1 Pambuyo payichi Davide anafunsa Yehova naku kamba kuyi, "Kodi ni ngayende kumuzida umozi wa Yuda?" Yehova anamuyanka enve, "Yenda pamwamba". Davide anakamba kuti, "nimuzinda uti wamene nifunika ku Yehova?" Yehova ana muyanka, "Ku Heberoni." 2 Chakuti Davide anayenda pamwamba naba kazi bake babili, Ahinomu waku Jezereli, na Abigele waku Kameli, ofelewa kuli Nabo. 3 Davidi ana bwela naba nyamata bamene bonse bana bwela nama banja yabo, ku muzinda wa Heberoni, kwamene bana yamba ku nkala. 4 Bamuna bochokela ku Yuda banabwela naku muzoza Davidi mfumu ya nyumba ya Yuda. Banamu uza Davide, "Bamuna baku Jebeshi Giliyadi bamu shika Saulo." 5 Chakuti Davidi anatuma batumiki bantu ba Jabeshi Gileyadi naku kamba kuli benve, "ndimwe bodaliska na Yheova, kamba kuti mwa onsea kuzi peleka kuli bwana wanu Saulo na kumu shika enve. 6 Manje lekani Yehova akuchitileni chokoma na cho'onadi. Naineso niza ku onesane ubwino uyu chifukwa wachita ivi vintu. 7 Manje pamene apo, lekani man ja ya u yalimbisiwe; nkalani olibika kwa Saulo bwana wanu afa, na nyumba ya Yud yani zoza ine mfumu kwa benve. 8 Koma Abineri mwana wa neri, olamulila wa Saulo bankondo, atenga Isiboseti mwana wa Saulo na kumuleta kuli Mahanaimu. 9 Anamupanga Isiboseti mfumu ya Gilayadi, Asher, Jezeli, Eframu, Benjameni, napali Isialyeli yonse. 10 Isiboseti mwana wa Saulo, anali na zaka fote pamene ana yamba kulamulila Isilayeli, ndipo analamulila zaka zibili. Koma nyumba ya Yuda ina konka Davide. 11 Pa ntawi yamene Davidi anali mfumu ku Heberoni pa nyumba ya uda inali na seveni na myezi sikisi. 12 Abineri mwana wa Neri, ndi anyamata Isiboseti mwana wa Sauli, anachoka ku Mahanaima ku Gibiyoni. 13 Yowabu mwana wa Zeruyana naba nchito ba Davidi anayenda naku bakumanya pa tamanda ya Gibiyoni. anankala pasni, Gulu imozi kupali yathamanda na bena ku mbali ina. 14 Abineri anakamba kuli Yowabu, "leka anyamata anyamuke na kuchita mpikisano pamenso ya bantu." 15 Pamene apo Jowabu anakamba kuti, "Leka ba nyamuke." PAmene apo anayamta ana nyamuka naku unjikana pamozi, Bali twelovu kuchokela kuli Davidi. 16 Aliyense muntu anatenga mpata kumbali yabo na kuta ya minkondo ku mbali ya opikisana babo, na kugwala pansi chapamozi. kwaicho malo yaja ya naitaniwa kuti "Helkati Hazzurimu, "wina" munda wa mukondo, " ya mene yali ku Gbiyoni. 17 Nkondo ina kula ya siku na Abneri na bantu ba Isilayeli bana gonjesewa pamenso yaba nchtio ba Davidi. 18 Bana batatu bamuna ba Zeruya banaliko: Yowabu, na Abishale, na Asaheli. Asaheli anali waliwirp ngati nyama ya kusanga. 19 Asaheli mwapafupi anapisha Abneri naku mu nkonkamo enve kopanda kubwelela munjila iliyonse. 20 Abneri anayanaga kumbuyo kwake na kukamba kuti, "ndiwe Asaheli?" anayanka, "ndine." 21 Abneri anakamba kuli enve, "pindamukila ku zanja mwina kumazele, naku gwila munyamata umozi naku tenga chida chake, "koma Asaheli sana pindamuke ku mbali. 22 Abina anakamba kuli Asahelo nafuti kuti, "Leka kunipilikisha. Nanga nichani kansi ufuna kuti nikulase ugwe pansi? Manje nanga nizakwanisa bwanji kuyimya nkope yanga kulangana Yohabi, mubale wako?" 23 Koma Asahelo anakana kupindamukila kwinangu, pamene apo Abina anamulasa mu tupi na kuja kobunta kwa lupanga, mwakuti lupanga uja unachokela kumbali ina. Asahelo anagwa pansi nafukelatu pamene apo. Pamene ali onse anali kufika pamene Asahelo anagwela nakumwalila, anaimilila chilili. 24 Koma Yohabu na Abishayi banapilikisha Abina. Pamene zuba inali kungena, banafika pa pili ya Ama, yamene ili pafupi na Giya ku museu waku chipululu cha Gibiyoni. 25 Bamuna baku Benjamini banasonkana beka beka pamozi pambuyo pa Abina naku imilila pamwamba pa pili. 26 Pamene apa Abina anaitana Yohabu naku mu uza kuti, "Nanga mupeni uza paya kosaleka? Nanga siuona kuti vizaipa posilizila? Papite ntawi itali bwanji kuti iwe u uze bantu bako kuti baleke kupilikisha babale babo?" 27 Yohabi anamuyanka kuti, "Monga mwamene Mulungu alili na moyo, ngati iwe siwenze wakamba icho, basilikali banga asembe bapilikisha babale babo mpaka kufikila kucha!" 28 Pamene apo Yohabu analinza mutolilo, na bantu bake banaleka kupilikisha Izilayeli, kapena kumenyana nafuti. 29 Abina na bantu bake bana enda usiku onse uja kupitila mu Alaba. Banatauka Yodani, kuyenda kuseni konse, mpaka kukafika ku Mahanahimi. 30 Yohabu anabwelela kupilikisha Abuna. Anasonkanisa bantu bake bonse, pamene panashota Asahelo na basilikali bokwanila nineteen ba Davide. 31 Koma bantu ba Davide banapaya 360 bamuna baku Benjamini pamozi bosogololewa na Abuna. 32 Banatenga mutembo wa Asahelo naku uika mumanda wa batate bake, wamene unali mu Betelehemu, Yohabu na bantu bake bana enda usiku onse, kunacha ndishi bafika mu Hebroni.