Mutu 10

1 Inabwela kupita mwakuti mfumu yaku Amoni inafa, ndipo Hanuni mwana wake mwamuna anapiyana ufumu mu malo yake, 2 Davidi anakamba kuti, "Niza muchitila chifundo Hanuni mwana wa Nahasi, monga batate bake banani chitila chifundo ine." Chakuti Davidi anamutuma banchito bake kuka simikiza Hanuni Zaba tate bake. Banchito anangena mu malo ya bantu baku Ammoni. 3 Koma basogoleli ba bantu bamu Ammoni banakamba kuli Hanuni bwana wabo, "Kodi uganizila kuti Davidi achitila ulemu batate bako chifukwa atuma bantu kuku tontonza iwe? Davidi sanatume ba nchito bake kuli iwe ku yanganila mu zinda, ku on elela, kwakuti apasule?" 4 Chakuti Hanuni anatenga banchito ba Davidi, naku bagela ndevu zabo, naku ng'amba vovala vabo paka kufikila kumatako yabo, naku ba tuma. 5 Pamene bana londolola ivi kuli Davidi, anatuma bantu kuba kumanya benve, chifukwa bantu benze bo chitisiwa manyasi kwambili. Mfumu ina kamba kuti, "Nkalani mu Jerico mpaka ndevu zika mele futi, ndipo munga munga bwelele." 6 Pamene bantu baku Ammoni banaona kuti ba zinukitsa kuli Davidi, bantu Ammoni anatumiza naku lipila Aramu waku Beti Rehobu na Zoba, twente sauzande asilikali ba mendo, na mfumu yaku maaka na bantu twente sauzande. 7 Pamene Davidi ananvela ivi, anatuma Jowabu naba silikali bonse bankondo, 8 Baku Ammoni bana bwela na kuimilila mumunyololo wa kondo po ngenela mumu zina wabo. Pamene Aremu waku Zoba na waku Rehobu, na bantu baku Tobu Maaka, ana zimilila beka pabili pbili mumunda 9 Pamene Jowabu anaonabankondo baimilila mumunyololo kumuyangana bali bonse kusogololo naku mbuyo, ana sanka bana ma Isilayeli Akaswili bankondo nakubaika benve kuli Aremu. 10 Bantu bonse bosalila bana ika mumanja ya Abishai mubale wake, ndipo anaba tuma mumalo mwake kumenyana naba nkondo baku Ammoni 11 Jowabu anakamba kuti, "Ngati ba Aremu nibo limba kuli Ine, ndipon iwe, Abishai, ufunika kuni pokolola ine. Ngati bankondo baku Ammoni baku limbila iwe, ndipo niza bwela kukupokolola iwe. 12 Nkala olimba, ndipo leka tionese ise kuti ndise olimba kuli bantu batu na muzinda wa Mulungu watu, chifukwa Yehova azachita chabwino kuchifunilo chake." 13 Chakuti Jowabu na basilikali ba nkondo bake bana kuka ku menyana na Aremu, ana kakmiziwa kutaba pamenso ba nkondo ba Isilayeli. 14 Pamene bankondo ba Ammoni bana ona kuti Aremu kuti bataba, na benve kuli Abisha naku yenda ku bwelela muzinda. ndipo Jowabu anabwela ku chokela ku bantu baku Ammoni naku ku bwelela ku Jelusalemu. 15 Pamene Aremu anaona kuti bana gonjesewa na Isilayeli, bana sonkana benve futi. 16 Pamene apo anaitana Aremu chigulu ku chokela kutali kupitilila mumana wa Eufurati. Anabwela ku Helamu, na Shobaku, Olamulila basilikali ba Hadarezeri, anayenda pasogolo pao. 17 Pamene Davidi ana uziwa ivi, analeta Isilayeli pamozi. naku choloka Jordan, naku fika ku Helamu. Aremu ana zikonsekela ku menyana na Davidi naku menyana naye. 18 Aremu anataba kuli Isilaye, ndipo Davidi anapaya seveni handiledi bantu babo ba ngolo na fote sauzande uyendesa akavalo. Shobaku olamulila bankondo babo anaba pweteka naku naku mwalila kwamene kuja. 19 Pamene mfumu zonse zernze banchito ba Hadarezeri anaona kuti a gonjesewa na Isilayeli ana panga mutendele na Isilayeli bana nkala banchito babo. chakuti Aremu anayopa ku tandilzila bantu baku Ammoni nafuti.