Mutu 8

1 Pamene apo Yehova anakamba kuli Moe kuti, "Yenda kuli Farao naku mu'uza enve, 'Yehova akamba ivi: "Leka bantu banga bayende kuti bakani pempeze in. 2 Uka kana kubaleka kuyenda, niza vutisa ziko yako yonse nama chule. 3 Na kamumana kaza zul nama chule. Viza bwela pamwamba naku zula na kuyenda mu nyumba yako, kuchipinda kwako, napa bedi pako. Viza yenda muma nyumba ya banchito bako. Viza yenda kubantu bako, mumauveni yako, na namo sakani zila mwako. 4 Na machule yaza kumenya iwe, bantu bako, na banchito bako bonse."" 5 Yehova anakamba kuli Mose, "Mu'uze Aroni, "Tambulula kwanja yako na nkoli pali nyanja, tumumana, mwamene manzi nkalila, na ku bwelesa ma chule mu malo ya Igupito." 6 Aroni ana anatambulula kwanja yake pamanzi ya Iguputo, naku ma chule yabwela pamwamba pa naku zula pa malo ya Iguputi. 7 Koma ba majiki bao bana bana chita mwamene banachitila na majiki yabo; bana bwelesa ma chule mumalo ya Iguputo. 8 Pamene Farao anaitana Mose na Aroni naku bauza, "Pmempelani kuli Yehova kuti enve achose ma chule pali ine na bantu banga. Ndiye pamene zibaleka bantu bayende kuti benve ba peleke nsembe kuli enve." 9 Mose anakamba kuli Farao, "Unga nkale namupata oniuza ine pamene ninga kupempelela iwe, banchito bako, na bantu bako, kuti ma chule bachosewe kuli iwe na muma nyumba na kunkala chabe mu mumana." 10 Farao anati, "mailo." Mose anati, "chinkale mwamene wa kambila, kuti uzibe iwe ati kulibe wina monga Yehova, Mulungu watu. 11 Ma chule bazachoka kuli iwe, muma nyumba yako, banchito bako, na bantu bako. bazankala chabe mu mumana." 12 Mose na Aroni banachoka pali Farao. Pamene apo Mose analila kuli Yehova pali vima chule vamene anabwelesa kuli Farao. 13 Yehova anachita monga Mose ana pempa: Ma chule banafela muma nyumba, makoti, na muminda. 14 Bantu banakolonganika pamozi, malo yaja yanali kununka. 15 Koma Pamene Farao anaona kuti amasuka, enve analimbisa mutima ndipo sana mvelele Mose na Aroni, monga mwamene Yehova anaba vamene azachita. 16 Yehova anakamba kuli Mose kuti, "Mu'uze Aroni, 'Tambulula kwanja yako naku menya kalukungu kali pansi , kuti inkale natu doyo pa malo ya Iguputo." 17 Bana chita sochabe. Ndiye pamene Aroni anatambulula kwanja yake na nkoli pansi pa doti. Tudoyo tona bwela pa bantu na vi nyama. Yonse kalukungu inankala natu doyo pa malo yonse ya Iguputo. 18 Ba majik bana yesa majik yabo kuti ba pange tudoyo, koma ina kanga. Chakuti kunali tudoyo mu bantu na nama. 19 Pamene ba majik banakamba kuli Farao, "Ichi nichi kumo cha Mulungu." Koma Farao anakosesa mutima wake, na kukana kuba mvelela. Chinali mwamene Yehova anakamba Farao azachita. 20 Yehova anakamba kuli Mose, "Nyamukani kuseni maningi na kuyenda kuimilila kuntangu ya Farao pamene akalibe kuyenda ku mumana. Mumu uze enve, "Yehova akamba ivi: "Basiye bantu banga bayende kuti bakani pempelele ine. 21 Ngati isuza baleka bantu banga kuyenda, ine inza tuma gulu yaba inzi kuli iwe, banchito vbao, na bantu bako, na muma nyumba yabo. Manyumba yaba Iguputo yazankala nama gulu ya inzi, ndipo na pansi pamene badyaka paza nkala ba inzi bambili. 22 Koma siku ija ine mwamene niza tengela malo ya Gosheni, mosiyanako mumalo mwamene bantu banga bankala, chakuti gulu yaba inzi si'iza nkalako. Ivi vizachtika kuti ndine Yehova ali mumalo yanu. 23 Ine niza faka chosiyanisa pali bantu banga na bantu bako. Cholangiza mpavu zanga chiza oneka mailo. 24 Yehova ana chita so chabe, na gulu ikulu yama inzi ina bwela munyumba ya Farao na munyumba yaba nchito bake. Yonse malo ya Iguputo, malo yana onogeka chifukwa cha gulu yama inzi. 25 Farao anaitana Mose na Aroni na kukamba kuti, "Yenda, Peleka nsembe mumalo yatu." 26 Mose anakamba kuti, "Sichabwino ise kuchita ivo, chifukwa nsembe zamene tima peleka kuli Yehova Mulungu watu nizo nyansa kuli ba Iguputo. Ngati tapeleka nsembe bwino bwino mumenso yabo yo nyansa kuli ba Iguputo, sibaza titema myala? 27 Iyai, nimasiku yatatu yo yenda muchipululu yamene tifunika kupanga, kuti tipeleke nsembe kuli Yehova Mulungu watu, mwamene anatilamulila. 28 Farao anakamba, "ine niza kusiyani muyende ndipo mupeleke nsembe kuli Yehova Mulungu wanu muchipululu. Ngati simuza yenda kutali. nipempeleleni ine." 29 Mose anakmba, "nika choka chabe pano, niza ma inzi yaku kuli Yehova kuti ma gulu yama inzi yaku siye, Farao, Banchito bako na bantu mailo. Koma usa chitenso boza paku salekelela bantu batu kupeleka nsembe kuli Yehova." 30 Mose ana choka pali Farao na kuyenda kupempela kuli Yehova. 31 Yehova anachita vamene Mose anapempela; na kuchosa magulu yaba inzi kuli Farao, banchito bake, pa bantu bake. kulibe nangu kamozi kanasala. 32 Koma pantawi iyi Farao ana limbisa mutima wake. ndipo sana baleke bantu kuyenda.