Mutu 7

1 Jehova anakamba kuli Mose kuti, "Ona, Nakupanga monga mulungu kuli Farao. Aroni mubale wako azankala mneneri wako. 2 Iwe uzakamba vonse vamene nizaku lamulila, Aroni mubale wako ndiye azakamba na Faaro kuti aba lake bana ba Isireli ba chokemo mu malo yake. 3 Koma niza mulimbisa mutima Farao, kuchoka apo niza langiza vounesa mpamvu zanga, zambiri zodabwisa, mu malo ya Egpto. 4 Koma Farao saza munvererani, kuchoka apo nizaika kwanja yanga pa Egpto naku chosa ma gulu yanga ya amuna omenyana, bantu banga, bantu baku Isireli, choka ku a,lo ya Egpto na vilango. 5 Egpto izaziba ati ndine Yehova nikafikiza kwanja yanga pa malo ya Egpto naku chossa ma Isireli pakati pao. 6 Mose na Aroni anachita sochabe; banachita monga mwamene Yehova analamulila. 7 Mose anali na zaka ayite, na Aroni anali na zaka ayite fili pamene bana kamba na Farao. 8 Yehova anakamba kuli Mose na kuli Aroni, 9 Pamene Farao azakamba kulli imwe `chitankoni cho dabwisana,' kuchoka apo uza kamba kuli Aroni, `Tenga nkoli yako uyi ponye pansi pal Farao, kuti isanduke njoka.` 10 Mose na Aroni banayendakuli Farao, naku chita vamene Yehova analamulila. Aroni anaponya pali Farao na nchito bake, naku bwela ku nkala njoka. 11 Pamene apo Farao anayitana ba nzeru na ng'anga zake. banachita monga majik yabo. 12 Mwamuna aliyense anaponya nkoli yake, chokonkapo nkoli inankala njoka. kom nkoli ay Aroni inamela njoka zabo. 13 Mutima wa Farao wenze unakosesewa anso sananvele, monga Yehova anakambila. 14 Yehova anakamba kuli Mose kuti, "Mutima wa Farao ni olimba, kuchoka apo anakana kubaleka bantu bayende. 15 Mukayende kuli Farao kuseni pamene azayenda ku manzi. muka imilile ku mbali kwa manzi muka mukumane, ndipo uka nyamule mumanja mwako nkloi yamene yenze ina sanduka njoka. 16 Mu'uze kuti, ` Yehova, Mulungu wa Ahebri, anitumma kuli iwe kukamba kuti, "Leka bantu banga bayende, chakuti baka niymike muchipulu. Namanje sumunanvele." 17 Yehova akamba kuti: chifukwa chaivi muzaziba kuti ndine Yehova. niza pana manzi yaka mumana ka Nile na nkoli ya kwanja yanga, kuchoka apo ka mumana kazankala magazi. 18 Nsomba zili muka mumana zizafa, naka mumana kazanunka. Ma Egpto sibaza nkwansia kumwa manzi yamu ka mumana. 19 kuchoka apo Yehova anauza Mose, "mu.uze Aroni," Tenga nkoli utambulule kwanja yako pa manzi ya Egpto, na pali kamumana, kamumana, ponkala manzi, na mosungila nsomba, kuti manzi yabo yankala magazi. chitanso kuti munkale magazi pa malo ya Egpto, namu vu gubu va planga na myala. 20 Mose na Aroni banachita vamene anabalamulila munlungu. Aroni ananyamula nkoli naku menya pa manzi yamu ka mumana, pamenso ya Farao naba nchito bake. Mumana onse unasanduka magazi. 21 Nsomba inali muka mumana infa naka mumana kanayamba kununka. Ma Egpto sibana kwanise kumwa manzi yamu musanje na magazi yenzeli pa malo ya Egpto. 22 Koma ba majik baku Egpto banachita monga benve na majik yabo. chokonkapo mutima wa Farao unalimba, nakukana nvelella Mose na Aroni, monga Yehova anakambila viza chitikila. 23 Kuchoka apo Farao anakoneka noyenda munyumba mwaka. sanafakeko na nzelu. 24 Ma Egpto bonse banakumba kumbali kwa kamumuna kuti bapeze manzi yokumwa, koma sibana kwanise kumwa manzi yamu kamunmana. 25 Masiku yali seveni yanapita kuchokela pamene anapandila pa manzi