Mutu 33

1 Pamene Yehova anakamba kuli Mose, "Yenda kuchoka pano, iwe na bantu bamene unachosa mu Iguputo. Yenda ku malo yamene nina panga ku lapila kuli Abrahamu, kuli Isaki, na kuli Yakobo, pamene nina kamba, niza pasa ku bana bobadwa kumbuyo kwanu, ' 2 Nizatuma mungeli kusogolo kwanu, nizaku choselani amu Kanani, Amorati, Hititati, Perezati, Hivazati, na Jubuzati. 3 Yendani kumalo, yoyenda mukaka na uchi, koma siniza yenda na imwe. chifukwa inu ndimwe bantu olimba mikosi. ninga kuonogeni imwe munjila." 4 Pamene bantu bana nvela mau chinaba vutisa, banalila, kulibe anavala vomu mukosi. 5 Yehova anakamba kuli Mose, "kamba kuli Isilayeli, 'ndimwe bantu bolimba mikosi. ngati naenda pakati panu inga nkale ntawi imozi, ninga kuonengeni, manje apa chosani vamu mukosi kuti ninga zibe vochita naimwe." 6 Sopano Isilayeli sinavale vokobekela ku chokela ku lupili ya Herobu kuyenda musogolo. 7 Mose anatenga tenti na kuimika panja kutalukila po nkala. Anaitana tenti po kumanila. Aliyense ana funsa Yehova kalikonse nali kuyenda ku tenti ko kumanila, panja ba campu. 8 Pamene Mose anali kuchoka kuptia ku tenti, bonse bantu benze ku yenda kuma tenti pongenela pao naku yangana Mose kufikila aka ngena mukati. 9 Pamene paliponse Mose aka ngena mutenti, kumbi yenze ku bwela pansi naku mulamulilanpo ngennela pa tenti, ndipo Yehova anali ku kamba na Mose. 10 Pamene bantu bonse bana ona kumbi yaimilila pongenela pa tenti, anali ku yamika naku lambila, mwamuna aliyense pongeneka mutenti yake. 11 Yehova anali ku kamba kuli Mose nkope na nkope, monga mutnu akamba na muzake. Pamene Mose anali kubwelela ku campu, koma wanchito wake Yoshwa mwana wa Nan, munyamata, anali ku salila mutenti. 12 Mose anakamba kuli Yehova, "Onani, mwankala mu kamba kwaine, 'Tenga aba bantu pa ulendo, 'koma zimuna nizibise bamene muzani tuma nabo. mwa kamba, "nikuziba na zinalako. naku peza mwai mu manso yanga. 13 Manje ngati na peza mwai mumaso yanu, nioneseni njila zanu kwakuti nkakuzibeni imwe na kupitiliza ku peza mwai mumaso yanu. kubukilani kuti ziko ili ni bantu banu." 14 Yehova anayanka, "kupezekapo kwanga ku zaenda ma iwe, ni zakupasa mupumulo." 15 Mose anakamba kuli enve, "Ngati kupezekapo kwanu siku yenda naise, musati chose pano. 16 Ndaba, chizazibika bwanji kuti napeza mwai mu menso yanu, ine na bantu banu? Sichiza nkala ngati muyenda naise kuti ine na bantu banu kunkala bosiyana na bantu bena bali paziko ya pasni?" 17 Yehova ana kamba kuli Mose, "nizachitanso ichi chamene wani pempa, chifukwa wapeza mwai mu manso yanga, niku ziba na zina." 18 Mose anakamba kuti, "Napapata ni oneseni ulemelelo wanu." 19 Yehova anakamba, "niza lengesa ubwino wanga kupita pa sosgolo pako, naku kamba zina yanga 'Yehova' pamenso pako. Niza chitila chisomo wamene niza chitila chisomo, naku onessa chifundo kuli iye wamene niza onesa chifundo." 20 Koma Yehova anakamba, "suzaona nkope yanga, chifukwa kulibe angone nkpoe yanga naku nkala namoyo." 21 Yehova anakamba, "ona, apa nipa malo panga; uzaimilila pa mwala uyu. 22 Pamene ulemelelo upita, niza kuika kumbuyo kuli mwala naku chingilza iwe na kwanja yanga kufikila nikapita. 23 Pamene niza chosapo kwaja yanga, ndipo uzaona kumbuyo kwanga, koma nkope suzai ona."