Mutu 32

1 pamene bantu bana ona huti Mose achedwa kubwela pansi kuseluka palupili, bana sonkana pali Aroni naku kamba kuli enve, "bwela utipangile mafano kopempeza kamene kaza yenda pasogolo patu. 2 Manje pali uyu Mose, mwamuna anati chosa mu malo ya Egipito, sitiziba vamene vachitika kuli enve."Manje Aroni anakamba kuli benve, " chosani mpete zamene zili pa matu ya bakazi banu, na matu ya bana banu bamuna naba bakazi, na kuzileta kuli ine." 3 Bonse bantu bana vula mpete za golide zinali pa matu yabo nakuleta kuli Aroni. 4 Analandila golide kuchokela mu manja yabo na kuyi pangamo na chopangila na kupanga mafano kopempeza muma onekede ya mwana wangombe. pamene apo bana kamba kuti, "izi ndiye mulungu zanu, Isreli, zina kuchosani mu malo ya Egipito. 5 Pamene Aroni anaona ichi, anamanga guwa pa sogolo pa mwana wangombe naku sindikiza vokamba vate; anakamba, " Mailo kuzankala madyelelo mu ulemu Yehova." 6 Bantu bana uka kusen siku yokonkapo naku leta nsembe zo shoka na nsembe zo pembeza. Pamene apo banakala pansi kuti badye no kumwa, naku imilila muma sangalo chamu chalo. 7 Kuchoka apo Yehova anakamba kuli Mose kuti, "Yenda mwamusanga, chifukwa bantu bako bamene una chosa mu malo ya Egipito bazi ipisa beka. 8 Baisiya njila mwamsanga yamene ninaba lamulila. Bapanga kamulungu kopempeza mu maonekedwe ya mwana wangombe nakuka pempeza. Bakamba kuti, "Izi, nimilungu zani, Isireli, zinaku chosani mu malo ya Egipito. 9 Pamene apo Yehova anakamba kuli Mose, " naba ona aba bantu. ona, nibantu ba ntota. 10 Apa manje, osayesa kunilesa. Ukali wanga uzaba shoka benve. Mwaicho nizaba onong benve. kuchoka apo niza panga ziko ya mpamvu kuchokela muli iwe." 11 Koma Mose anayesa kubwelesa pansi ukali wa Yehova Mulungu wake. Anakamba kuti, "Yehova, nichani ukali wanu che upyela pa bantu banu, bamene muna chosa mu malo ya Egipito na mpamvu zambili na mpavu zonse za kwanjia yanu? 12 Nchifukwa chani ba Egipito bazakabila, " Anaba sogolela kuba chosa muma ganizo nama ganizo yoipa kuti abapaye mu malupili nakuba ononga kuchoka pa menso yapa ziko ya pansi?" Bwezamo mutima naku chosapo chilango pa bantu bako. 13 Kumbukila Abrahamu na Isaac na Isireli, banchito bako, kuli bamene una lambila kuli iwe weka naku kamba kuli benve, "Niza panga ba mibadwo wako kuti bapake monga nenyezi mu mwamba, anso niza pasa kuli ba mibadwo bako malo yonse aya ninakamba, bazayi landila mwa muyayaya." 14 Kuchoka apo Yehova anachinja nzelu pa chilango chamene anakamba azachita pa bantu bake. 15 Kuchoka apo Mose ana zunguluka naku seluka lupili ninshi aimya magome yabili ya chipangano mu manja mwake. Magome yanali yolembeka ku mbali zonse zibili ku sogolo naku mbuyo. 16 Magome yanali nchito ya Mulungu eka, na vilembo vinali vilembo va Mulungu eka, vodindika pa magome. 17 Pamene Yoshua anamvela chongo cha bantu pamene bana punda, anakamba kuli Mose kuti, "kuli chongo cha nkondo mumsokano. 18 koma Mose anakamba, " sichongo chakupambana, anso sichongo chabo Gonjesa bantu, ni chongo chabamene baimba chne nmvela. 19 Pamene Mose anali kufika pa musonkano anaona mwana wangombe na bantu baivn. Anabwela akalipa maningi. Anataya magome kuchoka mu manja yake na kuya pwanya pansi pa lupili. 20 Anatenga mwana wangombe wamene bantu bana panga, ku ushoka, kuyitwa mosala, naku itila mu manzi. nakunpanga bantu bamu Isireli kuimwa. 21 24 Kuchoka apo Mose anakamba kuli Aroni kuti, "Bana kuchita chani aba bantu, kuti ulete ma chimo yakuli pali benve?" 22 Aroni anakamba kuti, "Musakalipe maninig bwana. Mubaziba aba bantu, mwanene ba kondela kuchita voipa. Banakamba kuli ine kuti, 'Tipangile Mulungu aza yenda pa sogolo patu. Manje pali uyu Mose, Muntu wamene anatichosa mu malo ya Egipito, sitiziba vamene vamu chitikila. 23 Mwaicho ninakamba kuli benve kuti, "Aliense alina golide, lekani ayivule; Banani pasa golide na kuitila mu mulilo, na kuchoka mwana wangombe." 25 Mose anaona kuti bantu bachita vamene benzo funa kuchita (Chifukwa Aroni anaba lekelela kupita malile, chinalengesa ba gudani babo kubaseka). 26 Mwaicho Mose anaimilila pongenela mumusonkano naku kamba, "Alionse ali kmbali ya Yehova, bwela kuli ine." Bonse ma Levitisi banamu zunguluka. 27 Akamaba kuli enve, "Yehova, Mulungu wa Isirelio akamba ivi: Lekani mwamuna alionse amange luoanga pa mbali pake na kuyenda kusogolo naku mbuyo kuchoka po ngenera kufika ngenera mu malo yonse ya musonkano, nakupaya mubale wake, munzake na onkala pafupi pake." 28 Ba Levite banachtia vamene Mose anabauza. Ija siku bantu fili sauzande banafa. 29 Mose anakamba kuli ma Levitisi, Mwaikiwa mu nchito ya Yehova lelo. chifukwa aliense pali imwe aimila mwana mwamuna wake na mubale wake, kuti Yehova anga kupaseni daliso. 30 Siku yokonkapo Mose anakamba kuli bantu, "Mwachita chimo ikulu maninigi. Manje niza kwela kuli Yehova, kapena nizachita chotetezela pama chimo yanu." 31 Mose anabwelela kuli Yehova anaku kamba, "Iyee, aba bantu bachimwa chimo ikulu na kupanga kamulungu ka golide. Koma manje, napapata bakululukileni machimk yabo; 32 koma ngati simuna chite ivo, mu nichosemo mu buku yamne muna lemba." 33 Yehova anakamba kuli Mose, "Ulionse achimwa kuli ine, Uyo muntu niza muchosa mu buku yanga. 34 Apa manje yenda, sogolela bantu bamene nakamba kuli iwe. Ona, mungeli wanga azayenda pa sogolo panu. Koma pa siku nizaba langa benve, nizaba langa pama chimo yabo." 35 Yehova anatuma chisongo pali bantu chifukwa benze bana panga mwana wangombe, wamene Aroni anapanga.