Mutu 8

1 Pasogolo pake Davidi anamenya Afilisti naku ba gonjesa benve. manje Davidi anatenga Metegi Amma muku lamulila Afilisti. 2 Pamene anabagonjesa ba Moabu na kupima bantu babo na myololo kuba gonesapansi padoti. anapima minyololo zibili kupaya, na munyololo ozula umozi kusumga ba moyo. chakuti Mowabu banankala ba nchito kuli Davidi na kuyamba kumu peleka musonko 3 Davidi pamene apo ana gonjesa Hadadeza mwana mwamuna wa Rehobu, mfumu ya zob, ngati Hadadeza anali kuyenda kabwezela ulamulilo kumu mana wa Yufurate. 4 Davidi anagwila kuli enve 1,700 ngolo na twente zikwi oyenda na mendo. Davidi ana masula pyendesa akavalo bonse, koma ana sunga bokwana benve kili kumi kumi ngolo. 5 Pamene alemu ba Damasika anabwela kutandizila Hadadezeri mfumu ya zoba, Davidi ana paya Makumi yabili zikwi Alemu Azibabo. 6 Pamene apo Davidi anayika chigilizo ku Aramu baku Damasiku, ndipo Alemu banankala ba chinto kuli enve nakumu letela musonko Yehova anamu pasa chigonjeso Davidi kuli konse anayenda. 7 Davidi anatenga chishango cha golide chinali pali wa nchito wa Hadadeza na kuzi leta ku 8 Yelusalema. Ku chokela ku Teba na Beroti, Mizinda ya Hadadeza, mfumu Davidi anatenga anatenga zambiri mikuwa. 9 Pamene Tou, mfumu wa Hamati, ananvela kuti Davidi agonjesa Asilikali bonse ba Hadadeza, 10 Tou anatuma Hadoramu mwana wake mwamuna kuli mfumu Davidi kumu posha enve nakumu dalisa enve, chifukwa Davidi ana menya na Hadadeza nakumu gonjesa enve, ndipo chifukwa Hadadeza ana menya nkondo na Tou. Hadoramu anabwela enve vintu va siliva, golide, na mikuwa. 11 Mfumu Davidi ana viyikapabali ivi vintu kuli Yehova, pa,ozi na siliva na golide kuchokela kuma ziko yamene ana gonjesa - 12 Ku chokela kwa Aramu, Mowabu, bantu baku Ammoni, Afilisti, na Amaleki, pamozi na vonse makatundu bana poka Hadadeza mwana wa Rehobi, mfumu ya zoba. 13 Davidi zina yake yenze yozibika pamene ana bwela muku gonjesa Alemu mu chigwa cha Sauti, na bantu babo bokwanila eyitini sausande. 14 Anaika vochingiliza ku zunguluka Edomu, na bonse bamu Edomu banankala ba nchito bake enve, Yehova anapasa chigonjeso kuli Davide kulikonse kwamene anayenda. 15 Davidi analamulila pali Isilayeli, anapeleka chilungamo na chiyelo kuli bonse bantu. 16 Jowabu mwana mwamuna Zelia anali olamulila asilikali na Yohasafati mwana wa Ahiludi anali kalembela. 17 Zadoku mwana mwamuna wa Ahitubi na Ahimeleki anali asembe, na Seraya anali olemba. 18 Benaya mwana wa Jejoyada anali ayangan ila wa kereti na Peleti, ndipo bana ba Davidi banali nduna zabo. ***Mbili zakale Ageliki omasulila na ku masulila kwasopano zilina ivi mu mbili 18:17 kwamene akulu kulu omashila: koma zakale Ahaberi zosunga anali azembe.