Mutu 5

1 Pamene apo mitundu zonse zamu Isilayeli zina bwela kuli Davidi ku Heberoni naku kamb a kuti, Ona, ndise nyama zako na bonzo. 2 Masiku yaku mbuyo, pamene Sauli ana fumu paisxe, ndiwe una sogolela Isilayeli bankondo. Yehova ana kamba kwaiwe, uza chita ubusa ku bantu ba Isilayeli, ndipo uzankala olamulila pali Isilayeli.'" 3 Chakuti basogoleli bonse ba Isilayeli bana kuli mfumiu ku Heberoni, ndipo mfumu Davidi ana pangana chipangano nao pamenso ya Yehova. bana muzoza Davidi mfumu ya Isilayeli. 4 Davidi anali na zaka satd pamene anayamba kulamulila, ndipo analmulila zaka fote. Mu 5 Heberoni analamulila Yuda zaka sevebni na mwezi sikisi, na mu Yelusalemu analamulila zaka sate fili pa bonse mu Isilayelu na Yuda. 6 Mfumu na bantu bake bana yenda ku Yelusalema kusiyana nama Jubuzati, bo nkala mu malo, ana kamba kwa Davidi, "Suza zabwela kuno koma chabe ku bwezewa na mpofu na vilema. Davidi sanga bwele kuno." 7 Ngankale choncho, Davidi anawilila malo yolimba ya Zayoni, yamene manje ni muzinda wa Davidi. 8 Pa ntawi ya Davidi anakamba kuti, " wamene aba menyana nama Jubuzati afunika kupita mu manzi yopidmula ndipo ulemala safunikila ku ngena mu malo." 9 Chakuti Davidi anankala milinga muja, na kuitana kuti muzida wa Davidi. Ana chingiliza mumbali monse, kuyambila mu malo kufikila mukati. 10 Davidi anankala wa mpavu chifukwa Yehova, Mulungu wa vonse, anali na enve. 11 Pamene apo Hiramu mfumu yaku Taya inatuma tumixs mitenga, kuli Davidi, ampala matambwa, amisiri. bana mangila nyumba Davidi. 12 Davidi anaziba kuti Yehova ana mukazikisa iye mfumu ya Isilayeli. ndipo anakwaza ufumu wake kamb a ka bantu bake Isilayeli. 13 Pambuyo yochokapo ku Heberoni Davidi naku bwela ku Yelusalemu, anatengelapo azi mai nini na azi kazi bena mu Yelusalemu, ndipo na bana bamuna naba kazi bobadwa kuli enve. 14 Aya ndiye mazina ya bana bobadwa kuli enve mu Yelusalemu: Shamwa, Shobabu, Natani, Solomoni, 15 Ibari, Elishuwa, Nefegi, Jafiya, 16 Elishama, Eliada, na Elifeleti. 17 Manje pamene Afilisti anavela kuti Davidi azozea mfumu wa Isilayeli, bana yenda bonse kumusakila enve. Koma Davidi anazivala naku yenda pansi milinga muja. 18 Manje ma Filisiti bana bwela naku tambalala muchigwa cha Refaimu. 19 Pamene apo Davidi anadunsa tandizo kuli Yehova. Anakamba kuti, "Kodi ningayende kumenyana nama Filisiti? Muza nipasa chigonjeso kwa benve?" Yehova ana kamba kuli Davidi, "Kamenye, Mo chimikizila niza kupasa chigonjeso pali Afilisti." 20 Chakuti Davidi ana menyana na Baalu Perazimu, nakuba gonjesa benve. anakambpo, "Yehova anapolika muli ba dani banga pamenso yanga ngati manzi yopulikila. "Chakuti zina yapa malo yaja yana nkala Bao Perazimu. 21 Afilisiti anasiya mafano yabo kuja, ndipo Davidi na bantu bake bana vinyamula kuyenda navo. 22 Pamene apo ma Filisiti bana bwela futi naku tambalalaso mochuluka muchogwa cha Rafaimu. 23 Chakuti Davidi ana sakila tandizo kuli Yehova futi, ndipo Yehova anakamba kuli enve, "Usa menyane kusogolo kwao. koma bazunguluke inkane kumbuyo kwabo na kutwaka kws benve kupitila ku basamu kuni. 24 Pamene ukanvela kuwayula muku menya kwamu pempo kupitila mu basamu mwamba mwamtengo ndipo menyani mwa mpamvu. Chitani ivi chifukwa Yehova pasogolo panu kuku menyelani asilikali ba Afilisiti." 25 Manje Davidi anachita monga Yehova anaba lamulila enve. Ana paya Afilisiti ku chokela ku seba kufika ku Gezeri.