Mutu 20

1 Ndiponso ni naona mungeli aseluka ku mwamba. Enze na fungulo ya ku chimugodi chosasila, ndipo enze na chi unyolo chikulu mu kwanja yake. 2 Ana gwila chilombo, njoka yakudala, ali mujelekezi, olo satana, naku mumanga zaka 1000. 3 Ana chiponya mu chimogodi chosasila, ana komako naku valikiza. Uku kwenze kuti asa pitilize kunama ma ziko mpaka pamene zina sila zaka 1000. Kuchoka apo, afunika amangusuliwe paka ntawi kang'ono. 4 Ndipo nina ona mipandu za umfumu. Benze nkalepo benze baja bana pasiwa ulamulilo oweluza. Nina onanso mizimu za baja bana duliwa mitu chifukwa cha umboni wa Yesu na pa mau ya Mulungu. Sibana pembeze chilombo olo fano ya cheve, ndiponso banakana kulandila chilemba pa mpumi olo pa kwanja. Bana nkala na umoyo, ndipo bana lamulila na Kristu zaka 1, 000. 5 Benangu bokufa sibana nkale na umoyo mpaka zaka 1,000 pamene zina sila. Uku ndiye ku ukisidwa koyamba. 6 Niwo dalisika naku yela ali onse wamene ankalamo mu ku ukisidwa koyamba. Kufa kwachibili kulibe mpavu pali aba. Bazankala ba nsembe ba Mulungu na ba Kristu ndipo bza lamulila naye zaka 1, 000. 7 pamene zaka 1000 zisila, satana azamumasula ku ndende yake. 8 azayenda kunamiza maiko mbali zonse za ziko lapansi-gog na magog kubaleta pamozi kuti bamenye nkhondo. bazankhala bambiri kwati ni dothi la mu manzi. 9 Bana yenda muziko na ku zunguluka musonkano wa bo kulupilila, mzinda okondeka. Koma mulilo unagwa kuchoka kumwamba kumwamba naku ba ononga. 10 Mujelekezi, anabanama, anaponyewa mu mumana wa moto na salifa, mwamene chilombo na mu neneli wa boza bana ponyewa. Baza zunzidwa muzuba na usiku muyaya. 11 ninaona mupando waukulu oyera na wamene anankhalapo. ziko lapansi na kumwamba kunathaba ulemelero wake, koma kunalibe malo yakuti zibisameko. 12 ninaona omwalira-ba mphamvu na opanda nchito-kuimilira pa mpando wa mfumu, mabuku yanaseguliwa. buku inangu inaseguliwa-buku la moyo. banthu bakufa banaweruziwa kulingana na zamene zinalembewa mu mabuku, kulingana na zinchito zawo. 13 nyanja zinachosa bamene banaferamo. imfa na hadesi zinachosa bakufa bamene banalimo, elo bakufa banaweruziwa kulingana na zamene banachita. 14 imfa na hadesi zinaponyewa mu nyanja ya muliro. uku nikufa kwa chiwiri- nyanja ya muliro. 15 ngati zina ya wina aliyense sinalembewe mu buku la moyo, anaponyewa mu nyanja ya muliro.