mutu 4

1 koma mumasiku yosiliza yazapezeka kuti pili ya nyumba ya YEHOVA iza konzewa bwino kuchila mapili yenango. izanyamuliwa pamwamba pa machulu, na magulu yabantu yaza tamangila kuli eve. 2 3 2 maiko yambili yazayenda nokamba kuti. ''bwelani, tiyeni tiyende pamwamba papili ya YEHOVA, ku nyumba ya mulungu wa yakobo. azati punzisa njila zake, ndipo tiza yenda mwamene apita. ''pakuti mu ziyoni lamulo izachokamo, na mau ya YEHOVA kuchoka mu yelusalema. 3 azaweluza pakati pa bantu bambili ndipo azasanka pa mayiko yambili mbili yakutali. bazapwanya malupanga yao kuya sandusa vo gaulila na mikondo yao kuyipanga mapwitika. ziko siyiza nyamula lupanga kunyamulila ziko inzake, olo kukonzekela futi nkondo. 4 5 4 koma, bazankala aliyense muntu pansi pa munda na pansi pa mutengo wake wa mpesa. kulibe wamene aza bayofya, pakuti kamwa ya YEHOVA wa makamu ya kamba. 5 pakuti bonse bantu bayenda, aliyense. muzina ya mulungu wake. koma tizayenda muzina ya YEHOVA MULUNGU watu kwa muyayaya. 6 7 8 6''pasiku ija''-uku nikukamba kwa YEHOVA -''niza sonkanisa pamozi bolemala na ku unjika ba kunja, abo bamene nina vutisa. 7 niza chinja bolemala kuba panga bosalako, na bopishiwa kunkala ziko yolimba, ndipo ine YEHOVA , niza ba lamulila pa pili ya ziyoni, manje na muyayaya, 8 koma kuli iwe wo yanganila vi beto, chulu cha mwana mukazi wa ziyoni-kuli iwe chiza bwela, ulamulilo wako wakudala uzabwezewa, ufumu wa bana bakazi ba ku yelusalema. 9 10 9manje, chifukwa chani upunda maningi? ninshi pungu wako amwalila? ninshi ndiye chifukwa chake kubaba kukugwila monga muzimai ali mukubala? 10 nvela kubaba nakusebenza nampamvu kuti ubale, mwana mukazi wa ziyoni, monga muzimai ali mukubala. pali manje uzayenda kuchoka mumuzinda, kunkala mumunda, na kuyenda ku babiloni. kweve baza ku pulumusa. kweve YEHOVA aza ku pulumusa kuchoka mu kwanja kwa badani bako. 11 12 11manje ma yiko yambili yasonkanila iwe; bakamba, 'lekani adesedwe; lekani menso yatu yamvele bwino pali ziyoni.' 12 sibaziba maganizo ya YEHOVA , kapena kumvesesa kukonzekela kwake, pakuti aba unjika monga mitolo ya tirigu yamene yakonzekelewa kupuntiwa. 13 13 nyamuka na kumpunta, mwana mukazi wa ziyoni, nizapanga nyanga yako kunkala nsimbi, nizapanga--------------------------------------------------. uza pwanya bantu bambili ndipo uza peleka chuma chao chosalungama kuli YEHOVA, chuma chao kuli MBUYE wa ziko lonse lapansi.''