Chapita 19

1 Kucita kwamaele kwacibili kunagwela pali simiyoni, banja pa banja. coloba cabo cinali pakati ka coloba ca Ayuda. 2 Coloba cabo cina Beersheba, Sheba, Moladah, 3 Hazar Shual, Balah, Ezem, 4 Eltolad, Bethul, na Hormah, 5 Simiyoni analinso na Ziklag, Beth Markaboth, Hazar Susah, 6 Beth Lebaoth, na Shauhen, Aya yanali mizinda fetini (13), kafakilako na mizi yabo. 7 Simiyoni analinso na Ain, Rimmon, Ether, na Ashan. Aya yanali mizinda fo (4) kafakilako na mizi. 8 Aya yanali pamozi, kufakilako na mizi yabo yozungulila mizinda kufika ku Baalath Beer (cimozi mozi monga Ramah ku mwela). Ndiyee cinali coloba ca simiyoni, banja na banja. 9 Coloba camutundu wa Simiyoni cinapanga mbali ya malo ya mutundu wa Yuda. Cifukwa gabo yamalo inapasa ku mtundu wa Yuda yanali yakulu kuli beve, mutundu wa Simiyoni unalandila coloba cabo kucoka pakati pa gabo yabo. 10 Maele yacitatu yanagwela pali Zebuluni, banja na banja, malile ya coloba cabo yanayambila pa Sarid. 11 Malile yanapita kuwamba kumazulo kwa Maralah na ku gusa Debbesheth; pamenepo yanakulila ku musinje unali pafupi na Jokneam. 12 Kucokela ku Sarid malile yanakonela ku mawa ku yenda kumawa kumalile kisloth Tabor. Kucokela uko yanayenda ku Daberth nakuyenda ku Japhia. 13 Kucoka uko yanayendela kumawa kwa Gath Hepher, na kuyenda ku Eth kazin; cokonkapo yanayenda ku Rimmon na kukonekela ku Neal. 14 Malile yanakonekela ku mpoto ku Hannathon na ku silila pa cigwa ca Iphtah Ei. 15 Ici cigabo kufakilako mizinda ya kattath, Nahalal, Shimron, Idalah, na Bethlehemo. Yanali mizida tyovv(12) pamozi, kafakilako mizi yabo. 16 Ndiye cinali coloba camutundu wa zebulun, banja na banja, mizinda aya, kufakilako mizi yabo, 17 Maele ya namba fo (4) yanagwela pa Issacah, banja na banja. 18 Malo yabo kafakilako Jezreel, Chesulloth, Shunem, 19 Hapharaim, Shion na Anaharath. 20 Inaikilako na Rabbith, Kishion, Ebez, 21 Remeth, En Gannim, En Haddah, na Beth pazzez. 22 Malile yabo yana Tabor, Shahazumah, na Beth Shemesh, nakusilila pa Yolodani. Tanali mizinda sikisitini (16) kufakilako mizi yabo. 23 Ndiye cinali coloba ca mutundu wa Issachah, kulingana na banja yabo - mizinda, kafakilako mizi yabo. 24 Maele yanamba faivi (5) yanagwela pali mtundu wa Asha, banja na banja. 25 Malo yabo kufakilako Helkath, Hali, Beten, Akshaph, 26 Allammeleki, Amad, na mishall, ku mazulo malile yanakulila ku carmel naku shihor Libnath. 27 Pamenepo yanakonekela kumawa ku Beth Dagon na kuyenda kutali monga ku Zebulun, na kuyenda ku cigwa ca Iphtah El, kumpoto ku Beth Emekina Neiel. 28 pamenepo yanapitiliza ku kabul ku mpoto. Ndiye inapita ku Abadon, Rehob, Hammon, na Kanah, kufaka ku sidon yaikulu. 29 Malile yanabwelela ku Ramah, nakuyenda kumuzinda wa malinga wa Tyre. pamenepo malile yanakonekela ku Hosah nakusilila panyanja, mucigabo ca Akzib. 30 Ummah, Apheki, na Rehob. Yanali mizinda yali twenti thu (22), kufakilako mizi yabo. 31 Ndiye cinali coloba ca Asha, banja na banja - mizinda, kafakilako mizi yabo. 32 Maele ya namba sikisi (6) yanagwela pali mutundu wa Naphtali banja na banja. 33 Malile yabo yayambila ku Heleph, kucoka ko Oak pa Zaanannim, kufaka ku Adami Nekeb na Jabneel, kufika ku Lakkvm; inasilila pa Yolodani. 34 Malile yanakonekela kumazulo kwa Aznoth Tabor na kuyenda ku Hukkok; inagusa Zebulun ku mwela, na kufika kuli Asha kumazulo na kuli Yuda kumawa kwa mumana wa Yolodani. 35 Mizi yobisamamo yanali Ziddim, Zer, Hammath, Rakkath, Kinnereth, 36 Adamah, Ramah, Hazor, 37 Kadesh, Edrei, na En Hazor. 38 Kunalinso Yironi, Migdal El, Horem, Beth Anath, na Beth shemesh. Yanali mizinda yali naintini (19) kafakilako na mizi yabo. 39 Ndiye cinali coloba ca Naphtali, banja na banja mizinda, kufakilako na mizi yabo. 40 Maele ya namba seveni yanagwela pa mtundu wa Dani, banja na banja. 41 Malo ya coloba cake kufakilako Zorah, Eshtaol, Ir shemesh, 42 Shaalabbin, Aijaloni, na Ithlah. 43 Inakilako na Eloni, Timnah, Ekloni, 44 Eitekeh, Gibbetho, baath, 45 Jehud, Bene Berak, Gath Rimmon, 46 Me Jarkon, na Rakkon pamozi namalo yakusogolo kucoka ku Joppa 47 Pamene malo ya mutundu wa Dani yanasoba kuli beve, Dani anamenya Leshem, kumenyana nayo, kuitenga nakuilasa napanga; kuitenga naku khalamo. Banapasa futi Leshem zina, kuitana Dani pa zina ya makolo. 48 Ndiye cinali coloba mutundu wa Dani, banja na banja, kufakilako mizi yabo. 49 Pamene banasiliza kupasa kwa malo monga coloba bana ba Israyeli banapasa coloba pakati kabo kuli Yoswa mwana wa Nuni. 50 Mwa cilamulo ca Yehova banamupasa muzinda wamene anapempha, Timnath Serah mu phili yaziko ya ku Eflamu. Anamanganso muzinda nakukhalamo. 51 Izi ndiye zoloba zamene Eliyaza wa nsembe, Yoswa mwana wa Nuni, naba sogoleli ba mitundu yabanja ya Israyeli yanapasiwa na maele pa shilo, pamenso ya Yehova, pakhomo ya cihema cokumanilamo. Ndipo anasiliza kupasa malo.