Mutu 18

1 Jeturo, wa nsembe waku Mdian, Mupongizi mwamun a wa Mose, ananela vonse vamene Mulungu anachitila Mose na bantu bake baku Isreali. Ananvela kuti Yehova anachosa Isreali mu Igupto. 2 Jeturo, mupongozi wa Mose, anatenga Zippora, mukzai wa Mose, pambuyo pakumutuma ku nyumba, 3 na bana bake bamuna babili; zina yamwana mwamuna umozi inali Geshomu, pakuti Mose anali akamba kuti, "Nankala mulendo mumalo achilendo." 4 Zina yawina inali Eliyeze, paukti Mose anakamba kuti " Mulumgu wamakolo banga anali tandizo yanga." ananipulumusa ku mpanga wa Farao." 5 Jeturo, mupongozi mwamuna wa Mose, anabwela na mwana mwamuna wa Mose na mukazi wa Mose muchipululu kwamene anali wasonkana papili ya Mulungu. 6 Anakamba kuli Mose kuti, " ine, mupongozi mwamuna wako Jeturo, nabwela kuli iwe na mukazi wak na bana bake babili." 7 Mose anayenda kukumana bapongozi bake, anagwada pansi. kuchoka apo anaba fyofyonta.Banafunsa pali umoyo wabo kuchoka apo banangena mumalo yokumanilamo. 8 Mose anauza bapongozi bake vonse vamene Yehova anachita kuli Farao nabantu bam Igupto kamba ka Isreali, navonse vovuta vabo vamene vinabagwela munjila, namwamene Yehova anaba pulumusila. 9 Jeturo anakondwela pavonse vabwino vamene Yehova anachitila Isreali, nakuti anapulumusa mumanja yaba Igupto. 10 Jeturo anakamba kuti, "Lekani Yehiva atandamike, pakuti akupulumusani kuchoka mumanja yaba Igupto na mumanja ya Farao, na kupokolola bantu munja yaba Igupto. 11 Manje naziba kuti Yehova nimukulu chila tumilungu tonse, chifukwa pamene ba Igupto anasunga ba Isreali mozikweza, Mulungu anapulumusa bantu bake." 12 Jeturo, Mupongozi wa Mose, anabwelesa voshoka nsembe ya Mulungu. Aroni na bakulu bonse ba Isreali banabwela kudya chakudya pamenso pa Mulungu na Mupongozi wa Mose. 13 Pasiku yokonkapo Mose anakala pansi kuweluza bantu. Bantu bana imilila mumbali mwake kuchoka kuseni kufika kumazulo. 14 Pamene mupongozi wa Mose anaona vonse vamene anachita kubantu, anakamba kuti, "kodi nichani chamene ukuchita ku bantu? nichani chamene iwe wankalila weka na bantu baimilila kuchokela kuseni kufika kumazulo?' 15 Mose anakmba kuli bapongozi kuti, " Bantu babwele kufunsa Mulungu mochitlia. 16 Ngati bali nakuangana, bamabwela kuli ine. Mina weluza pali muntu umozi na wina, nakuba punzisa monkalila mwa Mulungu na malamulo." 17 Mupongozi wa Mose ankamba kuli enve, vamene uchita sivabwino kwambili. 18 Uza zilemesa iwe nabantu bamene ulinao, chintu ichi nichachikulu iwe. Siuzakwanisa kuchita paiwe weka. 19 Nvela kuli ine. Nizakupasako maganizo, na Mulungu azankala naiwe, chifukwa ndiwe oyimililako bantu kuli Mulungu anso umupeleka vongan ngana vaba kuli iye. 20 Ufunika kubapunzisa va Mulungu na malamulo. Ufunika kubaonesa moyendela na nchito yosebenza. 21 Mopitilza, ufunika kusanka bantu boyenela bamuna kuchoka kubantu onse, amuna opasaa ulemu Mulungu, amuna achilingamo. Ufunika kubaika bo onelela bantu. bankale basogoleli bama sauzande, handiledi, mafifite, nama teni. 22 Bazayamba ku weluza mu nkani zonse zamasiku onse, koma nkani zovuta bazabwelesa kuli ine. kwa nkani zonse zing'ono, banga weluze bamene beka. Munjila iyo chizankala chapafupi kuli ine, anso bazanyamula chintu ichi ndi iwe. 23 Ngati wachita ichi, anso ngati Mulungu akulamulila kuchita so, kuchoka apo uzakwanisa kupilila, na bantu bonse bazakwanisa kupita ku ntumba okutila." 24 Anso Mose ananvela mau yaba pongozi bake bamuna naku chita vonse vamene banakamba. 25 Mose anasanka amuna oyneda mu Isreali na kubaitana basogoleli ba bantu, oyangani masauzande, ma handiledi, mafifite nama teni. 26 Ana weluza bantu moyenela. Nkani zovuta banazipeleka kuli Mose, Koma bene bana weluza nkani zosavuta. 27 Kucoka apo Mose analeka bapongozi bake bamuna kuyenda, na Jeturo ana bwelela kumalo yake.