Mutu 16

1 Bantu banayenda kchoka ku Elamu, na gulu yonse ya Isilayeli inafika muchipululu cha chimo, chilipakati pa Elamu na Sinayi, pasiku ya fifitini mumwezi wa chibili pene banachoka muziko ya Iguputo. 2 Gulu ionse ya Isilayeli ina dandaulila Mose na Aroni muchipululu. 3 Bana ba Isilayeli anakamba kuli benve, "Ngati chabe tenze tinafa mumanja ya Yehova malo ya Iguputo pamene tenze kunkala mumbali ya mapop yanyama nakudya buledi maningi. chifukwa wa tileta muchipululu ise bantu bonse kutipaya na njala. 4 Pamene apo Yehova anakamba na Mose kuti, "niza gwesa mukate kuchoka ku mwamba. bantu bazachoka nakutenga gao ya yao yasikuiliyonse kuti nibabonse ngati baza yenda mulamulo olo kapena sibaza yendamo. 5 Kuzabwela pa siku ya nambala sikisi, baza tenga kabili mwamene bantengela masiku yonse, na kuppika vamene waleta. 6 kuchoka apo Mose na Aroni banakamba kuli bantu bonse baku Isilayeli, "kumazulo muzaziba kuti ni Yehova anakuchosani mumalo ya Iguputo. 7 Kuseni muzaona ulemelelo wa Yehova, chifukwa anvela ku dandauka kwanu kuli enve. Ine na Aroni ndife ndani mwati dandaukila ise?" 8 Mose anakamba futi, "muzaziba ichi pamene Yehova akupasani nyama mumazulo na buledi kuseni okuta nabo. chifukwa amvela ma dandaulo yamene mumamu dandaulila. Aroni na ine ndise ba ndani? simudandaukila ise; koma Yehova." 9 MOse anakamba kuli Aroni, "Kamba kuli bantu bonse bana ba Isilayeli, 'bwelani pafupi na Yehova, chifukwa amvela madandaulo yanu." 10 Ina bwela kupita, pamene Aroni anali kukamba na bantu bonse bamu Isilayeli, bana yangana kuchipululu, na, onani, ulemelelo wa Yehova unaonkela muma kumbi. 11 Kuchoka apo Yehova ankamba na Mose, kuti, 12 "Namvela ma dandauko ya bantu ba Isilayeli. Kamba na benve kuti, 'Mumazulo muzadya nyama, naku kuseni muzazulisiwa na buledi. Kuchoka apo muzaziba kuti ndine Yehova Mulungu." 13 Ina bwela kumazulo nyoni zinabwela kuma zulo naku vininkila. Kuseni pamene mame yana zunguluka ponkala. 14 Pamene mamem yanasila, pamwba pa chipululu panali kantu kangono monga chipale pantaka. 15 Pamene bana ba Isilayeli banaona, banakambisana wina na wina, "nichani ich? sibana zibe kuti nichani, Mose pasanin kuit mudye. 16 Iyi ndiye lamulo yamene apasa Yehova: 'Alionse afunika kuyola vamene afunika kufya, omeli imozi ya muntu aliyense ya nambala ya bantu. Ndiye mwamene muzayolela, yolani vambili vakudya va muntu alionse muchihema chanu. " 17 Bana ba Isilayeli banchita vamene ivo. Bena banayo vambili, bena vingono. 18 Pamene bana pima na omeri yo pimila,baja bana yola vambili kulibe vinaslila, mbaja bayolu ving'ono sibanasube kalikonse. Alionse anayola vambili kukwa nisa vofuna vao. 19 Pamene Mose anakamba kuli benve, "Kusaseka aliyense usiyako pakana kuseni." 20 Koma benve, sanamu munvelele Mose. Benve banasiyako paka kuseni, koma inachokamvikusi na kununka. pamene apo Mose anakwiya na benve. 21 Bana kumana pamozi kuseni, Muntu aliyense analonga vambili vakudya vapa ija siku. Pamene ka zuba ina pya, inasungunuka. 22 Inachitika pasiku ya sikisi banayola kabili buledi. ma omeli ya bili ya mutnu slionde. bonse basogoleli bagulu banabwela na ku'uza Mose. 23 Anakamba nao, "Ndiye vamene Yehova akamba mailo na kupumula, sabata yoyela mukuleme Yehova. pangani vamene mufuna kupanga, pikani vamene mufuna kupika, vonse vosala vi ikileni pambali pakana mu mawa. 24 Ndiye anaika pambali paka kuseni, mwamene Mose anabauzila. Sivinaonongeke olo kupezekamo vikusi. 25 Mose anakamba, "idyani chokudya chija lelo, popeza lelo ni siku yopatulika monga sabata kulemez Yehova. elo sumu zavi peza mu munda, 26 Muzayamba kuyola mu masiku sikisi, koma siku ya seveni ni Sabata. Pa Sabata sikuza nkala mana." 27 Anso Inachitika kuchoka apo pa siku ya namba seveni bena bantu banayendaa kuyola mana, koma sibana peza kali konse. 28 Pamene apo Yehova anakamba na Mose, "muzakana kusunga malamulo na malembo yanga futi? 29 Ona, Yehova akupasni sabata. Pasiku ya sikisi akupasni buledi wamasiku yabili. Alionse waimwe afunika kunkala mumalo yake; kusapezke choka mumalo yake pasiku ya seveni." 30 Bantu bana pumula pasiku ya seveni. 31 Bana ba Isilayeli anaitgana vakudya kuti "mana" zinali zoyela monga mbeu ya mpasa, na kamvekedwe monga uchi. 32 Mose anakamba, "Ndiye vamene Yehova alamulila, lekaniomeli ya mana isungiwe na mibadwo ya bantu kuti bana banu bakaone buledi wamene nia kudyesani mu chipululu, pambuyo pokutulusani mu Iguputo." 33 Mose anakamba kuli Aroni, "Tenga poto ikamo omlei yamana, Isunge pamenso pa Yehoa, usungile ku mibadwo yanu. 34 Mwamene Yehova analamula Mose, Aroni anasunga pambali zonenela zachipango mu likasa. 35 Bantu ba Isilayeli andaaya mana zaka fote pakana banabwela kumalile ya ziko ya kanani. 36 Manje omeli niya namba teni ya Efa