Mutu 10

1 Yehova anakamba Kuli Mose Kuti, "Yenda kuli Farao, chifukwa na limbisa mutima wake na mutima zaba nchito bake. Ine nachita ivi kuti nilangize mpavu zanga pakati pawo. 2 Ine nachita ivi kuti muka buaze bana banu na bazukulu vintu vamene nachita, nayi sunga kuipa Egpto, anso na pasa zizindikilo zosiyana kulangiza mpamvu yanga pakti pawo. mwaso muzaziba ati ine ndine Yehova" 3 Kuchoka apo Mose na Aroni banayenda kuli Farao naku mu'uza Yehova, Mulungu wa Aheberi, akamba ivi: muzakana kufika liti kuzichepesa pamaso panga? Leka bantu banga bayende kuti bakaniyamike. 4 Koma ukakana kuba leka bantu banga kuyenda, nvela, mailo nizaleta vidiza pa malo yanu. 5 Viza vininkila pa mwamba pa malo kuti kulibe azayamba kuona pa ziko ya pansi. Bazadya vamene viza salako vina taba mu matalala. Vizadya mitengo yamene ikula mu munda. 6 Viza zula muma nyumba yanu, nayaba nchito banu, na binse bamu Egpto - chamene batate bako olo ba mbuya bako bakalibe kuonapo, kulibe kuchokela pamene bana nkala pa ziko ya pansi kufika siku ya lelo. kuchoka apo Mose anachokapo pali Farao noyenda. 7 Banachito ba Faro banamu'uza, "Uyu mwamuna azaleka kuti vutisa liti? Leka bayende baku Isireli kuti baka nimpempeze Yehova Mulungu wabo. ninshi simuona ati Egpto ya onongeka? " 8 Mose na Aroni banaleta futi kuli Farao, anakamba kuli benve," yendani kuli Yehova Mulungu wanu muka mu pempeze. Koma nibati bantu bazayenda?" 9 Mose anakamba, "Tiza yenda naba ngono batu naba kulu batu, bana batu bamuna na bakazi. Tiyenda na gulu ya vobeta na ng'ombe yatu, chifukwa tizankala nama dyelelo ya Yehhova. 10 Farao anabauza, Yehova ankale naimwe, nikaku lekani muyende natu ngo'no twanu kuyenda. Onani, mulina voipa mu nzelu zanu. 11 Iyayi! yenda, bamuna beka pakat pako, naku mpepeza Yehov, kaili ndiye vamene mufuna."Kuchoka apo Mose na Aroni bana ba pisha pamaso ya Farao. 12 13 Yehova anakamba kuli Mose, "Tambulula kwanja yako pa malo ya Egpto kuli vidiza, kuti vika menye malo ya Egpto na kudya vomela vilimo, vonse matalala yana sala." Mose ana tambulula nkoli yake pa malo ya Egpto, chokonkapo Yehova analeta chimpepo chaku mawa pa malo yaku Egpto muzuba monse na usiku. Pamene kunali kuseni, chimpepo chaku mawa chinaleta vidiza 14 Madiza yana yenda pa malo yonse ya Egpto naku zula konse, pakalibe kuonekako chikalile ku nyinji wa mutundunuyu wa madiza, kulibe yopalana ivi vizaka bwelapo nafuti. 15 Vina vininkila pa mwamba pa malo ya Egpto kuti kunankala na mudima. Vinadya vomela na vonse vi vipaso vaku mitengo yamene matalala yana siya. Pa malo yonse Egpto, palibe chamoyo chomela chinasala, olo mitengo na chomela mu munda. 16 Pamene Farao anayitana mwamusanga Mose na Arnoi naku kamba, "Nachimwa kuli Yehova Mulungu wanu naimwe. 17 Anso pano, nikululukileni ma chimo yanga pa ntawi ino, anso mupempele kuli Yehova Mulungu wanu achose infa pali une." 18 kuchoka apo Mose anachokapo pali Farao naku pempela kuli Yehova. 19 Yehova analeta chi mpepo cha mpamvu kumazulo nonyamula vi iza novi peleka mukamumana yama tete; sipanasale vidiza vili vons pa malile ya Egpto. 20 Koma mulungu ana limbisa mutima wa Farao, anso Farao sanabaleke ba Isireli kuyenda. 21 Kuchoka apo Yehova anakmba kuli Mose kuti, "Tambulula manja yako ku mwamba, kuti ku nkale mudima pa malo ya Egpto, mudima wa bii." 22 Mose anatambulula manja yake ku mwamba,ndipo kunali mudima bii mu malo ya Egpto masiku yatatu. 23 Palibe anali kuona aliyense; palibe anachoka pa nyumba pake masiku yatatu. mwaicho, kunali nkunkala ma Isireli kunali kotuba. 24 Farao anaitana Moe naku kamba kuti. "Yenda uka mu pempeze Yehova. nama banja yanu yanga yende naiwe, koma gulu ya vobeta na ng'ombe mu siye." 25 Koma Mose anakamba kuti, "Tivomelesenu tinkale navo peleka vo shoka kuli Yehova Mulngu watu. 26 Ng'ombe zatu zifunika kuyenda naise; kulibe bologodoili yonse izasala kumbuyo, chifykwa tizafunika kuti tika pempeza Yehova Mulungu watu chifukwa sitiziba vamene vo pempelezako Yehova mpaka tikafika kuja." 27 Koma Yehova anakosesa mutima wa Farao, anso sanaba lekelele kuyenda. 28 Farao anati kuli Mose, "choka pali ine! samalani pali chintu chimozi, kuti musaka ni onepo futi, chifukwa siku muzaka ana nfeshi yanga, muzakafa." 29 Mose anakamba kuti, "Iwe weka wakamba sinizaka onapo nfeshi yaku nafuti."