Mutu 17

1 Kuchoka apo Ahitopelo anakamba kuli Abisalomu kuti, "Apa amanje leka nisanke bazimuna bali 12000, ndipo niznyamuka naki tamangisa Davide usiku walelo. 2 Nizabwela pali enve pamene ali wolema nakufoka naku muduitsa manta. 3 Bantu bamene balina enve baataba, ndiye niza menya mfumu yeka. Nizaleta bantu bonse kuli iwe monga mukazi wofuna kukwatila aletewa kuli mwamua wake, ndipo bantu bonse bazankala namutenele pali." 4 Vamene Ahitopelo anakamba vina kondwelesa Abisalomu na bonse bosogoleli bamu Isilayeli. 5 Ndipo Abisalomu anakamba kuti, "Manje muyitaneni Hushi mu Arkuti, naye, tiyeni tinvele vamene azakamba." 6 Pamene Hushiri anabwela kuli Abisalomu, Abisalomu anamumasulila iye vamene Ahitopeleo anakamba nakufunsa Hushiri kuti, "Nanga tichite vamene Ahitopelo akamba? Ngati simwamene, tiuzevamene uza langiza." 7 Hushari anakamba kuli Abisalomu "malangizo yamene Ahitopelo akupasa ina ntawi siyabwino." 8 Hushari anapitiliza, "Uziba kuti batate bako na bantu babo bamuna nibankoma bolimba, ndipo nibo ukali, futi bali monga ka beeri kamene kapokewa tubana twake mu mumunda. Batate bako nibamuna bankondo,' sibazagona naba nkondo usiku walelo. 9 Ona, apa manje abisama mumugodi kapena mumalo yenangu chingachitike kuti bazimuna bako bapaiwa pakuyamba kwa kumenyana kuti aliyense wamene azanvelako azakamba kuti kujubiwa kwatenga malo pali asilikali bamene bakonka Abisalomu. 10 Chokonkapo nabo bailikali bochenjela bamene mitima zabo zili monga nkalamu, bazayopa chifukwa bonse ba Isilayei baziba kuti batate bako bamene ba mpavu, na bazimuna bamene alnaba nibo limba maningi. 11 Nikulanga kuti onse ba Isilayeli babwelel pamozi kuli iwe, kuchokela ku Dani kufikila ku Beershiba, mmga mwaunyinji wamu chi enga zamene zili ku nyanja, nakuti yende kunkondo weka. 12 Chokonkapo tiza bwela pali enve kuli konse kwamene angapezeke, naku muzunguluka monga mame yamene yagwela pansi. Sitiza siyako ngaklae umozi waba zimuna bake, kapena enve mwine wake, namoyo. 13 Ngati azabwelela mumuzinda, chokkonkapo ba Isialyeli bonse bazaleta ntambo kumu zinda naku donsela mu manzi, paka kunkale kulibe olo kamwala kangono kopezeka kuja." 14 Ndipo Abisalomu nabazimuna bamu Isilayeli banakamaba kuti, "Malangizo ya Hushari mu Akuti yaliko bwino kuchila ya Ahitopelo." Yehova anazoza kukaniwa kwa langizo ya Ahitopelo yabwino kuti aletete chionongeko pali Abisalomu. 15 Chokonkapo Hushari anakamba luki ZAdoki na Abiata wansembe kuti, Ahitopelo alangiza Abisalomi nabazi sogoleli bamu Isilayeli umu na umu munjila, koma namu langiza vinangu. 16 Manje apa yenda mwamusanga iye, 'Usiku walelo musagonele ku fordi ya Arabari, koma muyese ku tauka, ndaba mfumu izamelewa kufakako nabantu bonse bamene ili nabo."' 17 Manje Jonathani na Ahimazi benze kunkala ku kasupe ka Rogeli. Wanchito mukazi enzeli kuyenda naku bauza vamene benze kufunika kuziba, popeza sibenze kufunika, kuonewa kuti bayenda mumuzinda. Pamene utenga unabwela, chokonkapo nikufunika kuyenda kuona mfumu Davide. 18 Koma mwamuna mufana anabaona pa ntawi iyi nakuyenda ku uza Abisalomu. Pamene apo Jonatani na Ahamai bana chokako mwamusanga naku bwela kunyumba ya mwamuna wina mu Bahurimu, wamene anali na chisime pakomo apke, ndiye pamene bana gwela. 19 Mukazi wamuna uyo anatenga vovininkila vapa chisime naku gweselapo mbeu pamwamba pake, kuti aliyense asazibe kuti Jonatani na Ahimazi bali muchisime. 20 Bazimuna ba Abisalomu bana bwela kuli mukazi mwine wanyumba naku kamba kuti, "Ahimazi na Jonatani balikuti?" Mukazi anabauza kuti, "ba jumpe mumana." Pamene bana basakila konse konse naku sabapeza, bana bwelela ku Jelusalemu. 21 Chinfika kuti pamene batapita Jonathani na Ahimazi bana chokamo muchisime. Banayenda ku uza mfumu Davide; Banakamba kuli eve, "Nyamuka mwamusanga ujumpe pamwamba pa manzi chifukwa Ahitopelo apasa ivi na aya malangizo pali iwe." 22 Kuchoka apo Davide anayamuka na bantu bonse bamene banali naye, ndiye bana kuwoloka mu jordani. kufikila kucha kwa kuseni kulibe kapena umozi wamene anakangiwa ku wolololka Jordani. 23 Pamene Ahitopelo anaona kuti malangizo yake siya konkewa, anankala pali bulu yovala chonkalapoo nakuyenda kunyumba yake mumuzinda wake. Anakouza nyumba yake naku zimangilila anafa naku shikwa mumanda ya batate bake. 24 Kuchoka apo Davidenanabwela ku mahanimu. Koma Abisalomu anaoloka Jordani, enve nabazi muna bonse bamu Isilayeli bamene banali naye. 25 Abisalomu anafaka Amasa enzeli mwana mwamuna wa Jeta mu Ishimaliti wamene anayenda kuli Abigelo, wamene enzeli mwana mukazi wa Natashi na mulongo wa Zeruia, amai nake ba Yowabu. 26 Kuchoka apo Isilayeli na Abisalomu mu banankala muziko ya Giliyadi. 27 Chinachitika kuti pamene Davide anabwela ku Mahania mu, pamene Shobi mwana mwamuna wa Nahashi wochokela ku Rabai waba Amoniti, na Makiri mwana mwamuna wa Ammiel wochoka ku Lo Deba, na Bazillari mu Giliyaditi wochoka ku Rogelimu, 28 analeta vogoanapo navo vinikila, mabo nama poto, 29 na uchi, bata, mbelele, meleki, kuti Davide na bantu bamene alinabo badye. Bazimuna aba banakamba kuti, "Aba bantu balina njala, nibolema na luzu muchipululu."